Email a copy of 'DPP disown Bagus, Nankhumwa unveils Office as party candidate for Chikwawa Central' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP disown Bagus, Nankhumwa unveils Office as party candidate for Chikwawa Central' to a friend
United Kingdom UK) through British Peace Support Team (BPST) is supporting a national, election-focused command exercise that has brought together...
PAJATU YAWO IJA YOMAKATENGA ANTHU PA KUCHOKERA MZIGAWO ZOSIYASIYA AZITI KUNALI ANTHU AMBIRI WHAT ARUBBISH DPP
Koma ndiye msonkhano wa mafumutu kkkkkkkk koma dpp yathadi basi
DPP kuchedwa ndi ma strong holds anzanu pamene anzanu akukulowelerani ku chipinda
check msonkhano wa MIA PA MIGOWI
DPP is going out
Mafumu kuchuluka kuposa anthu wamba pa msonkhano, lorry ya chimanga yiripambalipo. Mafumu ena ali ntulo
Nankhumwa a Lomwe as regional vice chair, Mchacha a Lomwe as regional governor of the South. Kodi mitundu ina singapatsidwe maudindo kusiya a Lomwe? Yet you accuse MCP of being a party of people from Central region.
whats so special and different,if your brother wins an election as president you mean yourself will not have a position for the sake of other tribes.Stop the bluff man
koma Lundu adamema anthu kuti awiri akunenedwa apawa asadzawavotere…..chikwawa central ndiyovuta imafuna ma results….chiyambile democracy kulibe phungu adalamulilako two terms kunali bagusyu, fight, benadeta mlaka maliro lero kuli mwenye m’bale wake wa mia yemwe walephera sangawine Zaheer issa…koma owina uku ndi mai uja wachitukuko wa chipani chagwedeza paliponsechi cha UTM party mai Esnath Ross chidanti Malunga…mwana wa pa road…..moto kuti buuuuu
Unasiya chipani chabwino komwe unalindi udindo nkulowa chipani cha mbava komwe anthu akenso akukana. Iwe Bagasi nzeru zako nzopelewera ati. Ufyontenge, sunati.
Koma ndiyekunali anthu zide!!!! Chonchi?