Email a copy of 'DPP fight with Prophet Bushiri goes ugly: Cadets sing anti-Bushiri songs at Chinga funeral' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP fight with Prophet Bushiri goes ugly: Cadets sing anti-Bushiri songs at Chinga funeral' to a friend
During his address at the 51st independence celebrations, President Peter Mutharika unveiled three pillars namely integrity, patriotism and hard work....
Major 1 God Bless You, Pitilizani Ntchito Yabwino Yomwe Mukugwila,posatengela Zomwe Akuyakhula Anthu, Kodi A President Bwanji Mukhalangati Mwana Wakhanda? Mudzikula, Major 1 Simungamfike Or Mutadzola Mamina Amunthu Wamisala Aaraa.
Bushiri the Nyika Republic Billionaire the richest man in Nyasaland history God bless you keep own helping poor malawians they are not DPP children’s but God never punish people bcz of stupid leader we have todays God will fight for you.
Anthu otumikila mulungu, gwilani ntchito osayang’ana nkhope, ndi nthawi ya ana a Yehova, tinakusiyilani dzikoli kuti mwina zinthu ziyenda komanso mwakanika
Signs of the times
shame on you . kuzolowera kulemba macoomment otukwana basi. ndiye choncho mululungu asakwiye anthu amulungu ndi osapemphera onse kumangolakhula zofanana. lord have mercy on us
kodi bushili amalakwa chani? osafooka bushili go deeper
Guys
Chuma sitigawa ngati madzi. Even madzi amene timatha kugula. We should be very careful tikafuna kumusata munthu Chifukwa cha zinthu zomwe alinazo.
Tisayiwalw ndale za pamalawi sizikhala ndi nthawi.
Timayiwala kuti campaign anadusa pano ndi nthawi yokonza mavuto aziko lathu
Upulofeti anthu ayesa ngati business especially akangonena and zinthuzo nkutheka mmmmmmm nde kuti atiputa timachita kukagonera komweko kusata zozizwa ei
You think by disrupting funeral service then you’ll automatically win the 2019 elections. Kunali anzanu a UDF ankapanga zomwezi ali kuti lero, Mulungu simunthu, You’ll regret this. Watch this space.
Even if he stands for president ndiye vuto ndi chani. Agalu a DPP mumaona ngati amalawi mulipo nokha eti.
In my whole life I have never seen a SHAMEFUL Political Party as DPP.