Email a copy of 'DPP infighting: Nankhumwa whipping up hatred against Chaponda' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP infighting: Nankhumwa whipping up hatred against Chaponda' to a friend
As the year winds up, the Soul Savers Church at area 25 in Malawi’s capital Lilongwe has organized a night...
Olo munyoze oro mutukwane atumbuka ndi inu ochedwa ochewa mwanyanayo basi , ngati mwanya ndi 50+1 muona
amane akukutumaniyo wanya nayo kale mumati mutenga boma ndi timademo tanu mwayerara
akanakhala kuti he is doing it good faith, he would have taken his suggestion to the president or Chaponda himself.koma chokha chongopita ku media shows that he wants the position and he knows kuti anthu atukwana chaponda.. Achoke ndi iyeyu Nankhumwa nkhope ngati Bilisi
Asakane ufiti ndiwache many of us knows that he is the one behind many Gurus downfall he has his own devilsh scheme tool ambitious this Chisitu Guy they underestimated him but alas a crocodile
Tikufunadi achinyamata koma osati mbuli yachuma, yakaduka komanso yatsankho ngati ichi mukuti Nankhumwachi
Chaponda sangaime pa Nankhumwa. Even in his constituency, he is so loved by Many
Chaponda leave our dear Nankhumwa alone, he has done god as the Leader of the House. Congrats for all the suc
cess during the recent parliamentary deliberations
EDITORIAL……. CHAPONDA SHOULD STOP BLAMING OTHERS FOR HIS OWN MESS: LET HIM PAY THE PRICE FOR HIS ARROGANCE, GREEDY. QUICK FACTS • George Chaponda was chased in his own constituency by angry constituents • George Chaponda is one arrogant DPP officials who is not liked by many • George Chaponda was found in the wrong side by parliamentary inquiry committee • George Chaponda was arrested by ACB for his own wrong doings • George Chaponda is going under trial by the courts in Malawi George Chaponda should stop blaming some officials in the ruling DPP and others for his own… Read more »
Ukulemba ngati Nankhumwa amene!
Ukamva kuti DPP ndi ya dzigawenga anyamata ake ndi amenewa.Olo mtolankhani Chimakupa chokha makofi.Kondwani Nankhumwa the Mafia.
Zamanyazi a kondwani! tinkaona ngati poti ndinu onyasa ndiye kuti muli ndi nzelu koma ayi ndithu.Munanyasa ndi mmutu momwe.Osangothokoza kuti munalawira unduna uchifwamba
zamanyazi a kondwani! tinkaona ngati poti ndinu onyasa ndiye kuti muli ndi nzelu koma ayi ndithu.Munanyasa ndi mmutu momwe.