Email a copy of 'DPP justifies political violence against MCP at Chilembwe memorial: ‘We’re ruling Malawi’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP justifies political violence against MCP at Chilembwe memorial: ‘We’re ruling Malawi’' to a friend
The Journalists Union of Malawi (JUMA) has slammed some "invisible political machinations" behind the action by the Malawi Revenue Authority...
LETS AWAIT 2019
Kodi 2019 kulidi chisankho? Nanga opposition sikupeza munthu weniweni wodzapikisana ndi APM bwanji? Wasting time commenting on Nyasa instead of going in the field to meet voters. Munamuona bwanji Nankhumwa kogawa zinthu kuja? Ngakhale msonkhano wa Chakwera ku CR ungafike pamene paja? DPP ikutenganso bomali 2019 because opposition ndi mbola zokhazokha.
what shows here is just primitive politics there is no territory for any party , every part is free to go anywhere we are in a Multiparty system of Government this total no sense and not accepted DPP must stop this with e mediate effect
Munthu zitamukanika amathamangira kuopyseza azake,Atakhala President wanzeru akuyenera kudzudzula makhalidwe oyipawa komaso zomwe alakhula a Kasaira zukutsimikizira kuti DPP ili ndi anthu opanda nzeru okhaokha amene mbongo mwawo muli mamina okhaokha.Kodi aliyese atati azipanga zimenezo ndiye kuti kukhala nkhondotu chifukwa a MCP nawo Ali ndi Madera awo.
Dzikoli ndi lathu dzikoli ndi lathu koma pitalayu wawononga afe afe pitalayu wawononga
dzikoli ndi lathu dzikoli ndi lathu koma mtchona uyu wawononga afe afe mtchona uyu wawononga
Dpp is a walking devil that must be erased from Malawi, its leaders and most supporters are educated salvages good at stealing and killing, they are devils puppets who clad in devils regalia full of ignorance. There secretary general Francis Mphepo and their party leader are idiots who don’t know what life entails, they are cowards who din’t learn a lesson from their mose walero death. Let them know cardiac arrest redeemed us from Bingus brutality and this time the same cardiac arrest will redeem us from this dull professor and your stupid Kasairas who always back up on every… Read more »
Komansoo awa akuti a mmc ndinu wotani,or manyazi mulibe??why do you always talk zopusa against MCP..???be civilized babaaa..try to be human sometimes,mmmxiieww.
Oh, but I remember during campaign Kanyoza a DPP cadet was driving a car with flash light on APM’S convoy , that time they were not beaten though they were lving in denial that Bingu was no longer the president.
Chakwera has never done that.
IF IT WAS A CHURCH FUNCTION, WHY ISIT THAT DPP SUPPORTERS WERE PUTTING IN PARTY UNIFORMS. YAMBANI MWACHOTSA CHISOSO M’MASO MWANU MUSANAYAMBE KUKANGANA NDI ENA.
INU KU CENTRAL REGION SIMUMAPITAKO? KUPUSA!!!
Mulungu akufuna kuti Mutseguke Maso amalawi, Don’t ever do the same mistake in 2019. Malawi suppose be a milk & honey right nw!!!!