Email a copy of 'DPP primaries start with battle of ex-CEOs: Rosemary Mkandawire defeats Bruce Munthali in Mzimba North' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP primaries start with battle of ex-CEOs: Rosemary Mkandawire defeats Bruce Munthali in Mzimba North' to a friend
President Peter Mutharika has taunted the civil society organisations (CSOs) which organised nationwide anti-government protests on September 21 which he describe...
Quota system is targeting the north. If Lomwes were intelligent would there be such an outrageous system against them? A Rosemary muganinizirepo apa. You don’t love the north. Bruce Munthali ndi nkhungu. He is a well known crook who once converted to Islam just to appease Bakili wotukwana.
My boss, congratulations koma chipani mwasankha aaaaaa mungwa chigada bolani mukanaima independent osati chipani cha mbamva zimenezi inr mulibe voti yanga
Chonde Mayi mutsaapatse moni abambo awo.. mungawone chinameta khanga mupala….
Mukayan’ganatso kumbala mulakwitsa ..mungowauza masuppoter anuwo kuti mukhala pambali… kuatalikira
Congrats masteni you have done a lot kumeneko including building a stadium for the people ..I am only worried of the choice ya chipani mwajoyina… bola independer yikanazagwira chaka cha mawa
Ngati mukuti mwayamba bwino mdala mnthali akudandaula chani?Kuvotera DPP kukhala ngati kutembeleredwa,,,kkk
Kikiki. From Toyota Malawi/mdf cashgate to politics? Just for protection. Mudzayankha mafunso ku koti posachedwa iwe mbava.
Mzimba North is blessed with ex-CEOs: Munthali, Mkandawire, Nyaloge, Gondwe etc
At least we are seeing mature politics and organised primaries by DPP osati izi za chipani cha ng’onazi ayi
What’s the difference?
Wakhawula pera Bruce, uluchitapo vichi iwe kuti ukwezge ulimi wahona kuno? Watinyoza vilimika namwaka kutigula hona masensi ndalama ukwiba. Khawu
Akutani kodi ameneyo yekhayekha, akumumeta? kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk
Madala team mukumva bwanji mdala mzanu akudandaulatu apa. DPP ikupitilira kugawikana ndiye ithelatu.
Cadet tsekula pakamwa tikumve.