Email a copy of 'DPP, rights activists condemn Chief Lundu’s ‘reckless’ attack on Prophet Bushiri church' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP, rights activists condemn Chief Lundu’s ‘reckless’ attack on Prophet Bushiri church' to a friend
Malawi President Peter Mutharika has appointed two new High Court judges. High Court of Malawi and Malawi Supreme Court of...
olo kuwona majekete akewo, umangodziwilatu kuti ndiwodwala mutu wawukulu!!!!
Chief cool down
Kkkkkkk a stupid person and a party can distance itself but we all know where that stupid rally was organised by dpp so dont put yourself away from lundu……who gave lundu the podium? Mwasowa pogwira abale akakhala madala akutukwana kkkkkkkķkk…..akuti stupid critics…..
Lundu ndi munthu mmodzi amene amagwiritsidwa ntchito ndi chipani cholamula cha DPP, kumbukilani pamalilo ena ake ndiyemweyu emwe ananyoza chakwela koma boma linakhala losangalala kwambili ndi zolankhula zake ngakhale panali pamalilo,lelo ndizimenezi wayamba kunyozana ndi amipingo– samala iwe lundu ndi chipani chakocho, ulibe udindo omuweluza munthu kapena mpingo ntchito imeneyo umusiile amene anakulenga iweyo…Zopusa basi
Mfiti yaikulu iyi…Kukonda kunyenga tiwana..
Mapazi ache!
Tamuoneni nkhope yacheyo!!!
Komatu mfumuyi kuletsa kupemphera yapala, koma nonse mukudziwa kuti kikunena zoona….. Munthu uyu siwa Mulungu… Mkuluyu akulowa ndale ndi Chris Daza,, mkuluyu ndiwa sataniki zoona…
Forgive him. He is a sick man. His utterances are under the influence of drugs.
Mfumu ikamalankhula mbwelera chonchi, dziwani kuti imfa yake ili pafupi
Why is this so called chief given the podium to utter such careless and reckless remarks? He is usually under the influence of alcohol obviously. Chiefs are supposed to be unifying characters and not dividing people this way. It is very comforting that the ruling DPP has distanced itself from such careless remarks. I am not a Bushiri fan or follower but surely this utterance from this chief is nonsense. Someone must stop giving him the podium, for heaven’s sake!
kenaka timva kuti azipani zinazi musadzachititse msonkhano ku dera langa kkkkk mafumu amasiku ano amenewo ukuona ngati DPP ikupatsa kenakake walemba mmadzi