Email a copy of 'DPP's field marshal Ben Phiri tells Salima, ‘Mutharika deserves another term’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP's field marshal Ben Phiri tells Salima, ‘Mutharika deserves another term’' to a friend
SThe Standard Bank Be More Race is back with stakes raised and some major changes and surprises compared to the...
“APM treats all Malawians equally. He distributes development projects evenly across the country irrespective of tribes or regions”….I like this statement but I strongly disagree!!!! Action speaks louder than words Ben Phiri!!! Nenani zina otherwise nepotism and regionalism is the whole mark of the DPP government. Most articulate Malawians cannot differentiate between DPP and Mulhako!!!
pamene tinkavotera kuchotsa Tambala wakuda muboma mu 1994 tinkafuna ufulu, chitukuko kuti dziko lathu likhale lopita patsogolo. koma chosaziwa a Malawi ena anakuwa “tivotela wakuba yemweyo” monga mwachikhumbo cha a Malawi pofuna kusintha zinthu anavotela wakuba. Wakuba anabwera ndi akuba anzake omwe akutilamulila mpaka pano. Kuba kunayamba 1994 pano kwangokhala ngati chikhalidwe cha a ndale ndi akulu akulu a m’boma. Anthu wamba umphawi wokhawokha. Pano Tambala wakuda akumveka kuti kokoliko kwacha. A Malawi pano tivotela Tambala wakuda basi. Tambala abwelere akonze dzikoli. MCP 2019 Boma Boma Boma Kwacha Kwachaaaaaaaa
Lol! Maloto achumba , constituency imeneyo anapanga lease Kaphamtengo Yona, a Jumbe ngati akufuna ku parliament akayimile ku Dedza, DPP is not ticking in this country, the political landscape has changed.
lets try new fellows, Malawi is failing.
za ziiiii
The talk of our field marshal. Bravo brother Phiri. Mumatiimirira ife achinyamata. I remember you in 2014 in mzuzu at Mimosa hotel taking board steps in uplifting our blue colour. You r irreplaceable and we need your services more than ever now that people r too brind to see meaningful dev under difficult circumstances during this term of APM. Akadakhala ena aja akadatani, azungu andiuza kuti! Enawa apanga phokoso chabe popeza akudya nageya koma mzeru zoyendetsera dziko alibe ndiimodzi yomwe. For once let’s work hard to achieve our needs.
Uzeleza pera za zi kkkkkkkkkkkkkk !
Shaaaaa another term for what black out and generator again fotseki we have no time as Malawians to that forget a second term to Muthalika.
In nyaudomain you should also flexi the muscles just like the local nyau dancing phiris gunning for MCP.
IT’S ONLY ONE YOUNG
TALENTED YOUNG MAN WHO
CAN TAKE OUR MOTHER MALAWI TO GREATER LEVEL
BUSHIRI AKA MAJOR 1
WITH YOU GUYS MALAWI
WILL NEVER EXPERIENCE A
SIGH OF RELIEF.