Email a copy of 'DPP's 'sesa, sesa’ orator Saonda in bribery scandal' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP's 'sesa, sesa’ orator Saonda in bribery scandal' to a friend
Newly appointed Nico Life Chief Executive Officer Eric Chapola had a rude awakening on Sunday evening when he was slapped...
Saonda ndiwoyerekedwa, greedy & a crook!
search me
Jeffrey mumalimbana naye chisoni msiyeni Dada waku nkhotakota adyerere ndale za Dpp ndimzimayi olimba ameneyu kugwetsa makhang’a pa ndale kaka Dr chilumpha(former VP),komaso Fahad Assan amene anali senior minister nthawi ya amai simasewera ayi muzimupatsa ulemu,moreover she is from central region… Dada musafoke mupitirize kugwira ntchito molimbika ndimokhulupirika
kodi inu a dpp mukamapereka udindo kwa munthu mumafuna chikhale chowopsezera?pano saonda akuopseza anthu ndipo nthawi zonse amayankhula kuti iye amafika pali ponse moti akuti ngakhale Peter amanvera iye.Dpp thandizani anthu omwe anavota saonda watikwana
Mjcentral, you are right. Awaombe kumene. Amene muli madolo tawadyereni amwenyewa. Akutiyenjeza agalu amenewa. Wabwera bhooo sesa sesaaaa
I am not surprised at all. Activities such as Saonda’s are perfectly normal in DPP.
As for Jeffrey, my advice is for her to get out fast. Positions like hers are for DPP’s sacred cows from the Lhomwe belt or, if anything at all, from South.
DPP paulendo
Akhakhakha, ikanakhal MCP bwezi muli ng’we-ng’we-ng’we apa….
shupitiiiiiiiii!
Kodi amwenyewo amafuna chiyani kwa President wathu wokondeka?? Kuzolowera katangale basi….. Azikudyerani choncho.