Email a copy of 'Drama as fan is seen peeing on the goalposts' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Drama as fan is seen peeing on the goalposts' to a friend
Many times God’s children have been in situations that do not look good at all. These are some of the...
Tionanana loweruka
Tiona Saturday kuti azatan!!
Koma ku Malawi ndiye tikuyaluka nazo izi!!! A wanderers kukhulupilira nyanga too much. last time anapaka mafuta a nkhumba ku Blantyre. Anyway flames yathu sizapita patali.
muti in action kkkk
KASOVANI IFE ON SAT. FINALS PANO ILI MMANJA 5MITA WETHER WE LOSE, UMBONI WA ANANUUUU? KAGWEREN UKO. MUKATENGE ANU, ENA MUPATSE FLAMES (SIIDZAMVA) A BAD CARPENTER BLAMES HIS TOOLS. KKKKKKKKK! UKO KUNALI KULIRA KWA NDAN PAJA?
MIKODZO IMASULUTSATU SIMASEWERA, USALIRE NEBA IWE PA EASY PA THABWAPO, WAIT UONERE BALLS YOKOMA SI ZA MADUNYU ANU AJA, MPAKA RVG ANATHAWA GAME YANU!
Uchitsiru. I can’t support timu ya anthu okodza ndikunyera mu ground. Nyerere zonyera pali ponse.Savages!!!
Ma steward akwathu kuno sadziwa ntchito yao. I dont know who trains them, amaonera mpira pomwe a maiko ena amayang’ana ku ma stand koma athuwa maso tudzu mground akachinya uwaona akujowa nawo kkkk I dont think they will write any report poti izi sanaone pomwe zimayambira for Vales is a total shame
Hahaha kuli Nyerere ku manoma! Simunati mumva m’bebe
Kodi anakodza kapena ayeserera kukodza?
Mmmmmvkoma mpirawu ndiye wafikadi povuta
Apolice kumangoyang’ana??????????