Email a copy of 'Ex-Miss Malawi UK to host fundraiser for flood-stricken Malawians' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Ex-Miss Malawi UK to host fundraiser for flood-stricken Malawians' to a friend
Malawians living in diaspora and friends of Malawi have been asked to make donations which will go directly to helping...
Mmpaja munayambira kulandila ma donations, ka dziko kang’onong’ono kukukanikani kutukula. Chifukwa cha kuba anthu in a M’boma. Simunganizila anthu ayi koma munthumba mwanumo…
Ndalama zimenezo akadya ndi atsigoleli a malawi. Osati ma victim.
mukufuna kudyera anthu agalu inu
Kukongola ukamakhala kunja, bwerera kwanu iwe
mpaka big walk ? too late this is a crisis , nzofunika kungosonkha zovala zofunda anthu tithandizike, ma shift anthu apita liti , am sure they got old clothes etc to help sustain us. yosonkhayo ndakaika aliyese akuopa floodgate ndalama anthu ali nazo atha kusonkha koma nkhawa zingapite mwa acina lutepo etc anthu amangile mipanda mma line mu.
very beautiful girl !! keep on remembering poor people in your land not only pamavuto
may almighty allah bless u