Email a copy of 'Ex-MP Bernadetta Mlaka Maliro to release music album July' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Ex-MP Bernadetta Mlaka Maliro to release music album July' to a friend
We have a crisis situation in our country - the clash of jurisdictions, a feud between Members of Parliament and...
Kutha kwa ma plan. Ku Parliament kukangolawako ndi timbiri tosakhala bwino. Kaya zinali zoona kapena ayi mukudziwa ndi inu eni ake. By the way you are supposed to be called Bernadetta Maliro not Bernadetta Mlaka Maliro,, kwanu nkuti mayi? Olo musaike Mlaka anthu akudziwa kuti ndinu mkazi wa Mlaka. Pa Mlakapo muikepo dzina lanu lapakati la amuna anuwo lisiyeni sinanu. Mukakondwa kwambiri mutha kumangoti Mrs Maliro,, timaterotu.
Welcome ngati chili bwino tidzagula. A point of order since 2010 u didn’t have time to go to studio. What made you busy popeza ngakhale nthawi yomweyo kunalibe parliamentary deliberations inu kumudzi simumapezeka nor kumveka kuti mwina munali ku social activities, meetings hence people kicked u out. Nenani zoona kuti pano ndilibe chochita chooneka ndiye ndamukumbukira Mulungu mukuimba. Siinu nokha who forget God when blessed. May be this should be your lesson that in everything u should praise God as 1 Thessalonians 5: 18
sopano ndiye zikhala bwino. keep it up.
yes try and error
KKKKKkkkkkkkk!Plan B!
The level of communion determine the level of authority, well Mama i love be commune to God your level of authority in music industry will such greater and greater and i prophesy it to happen so may testify. Dont go for money but for your ministry and money will follow you, the bible seek you first the kingdom of God and His righteousness and all shall be added unto you (mathews 6:33)
your blessed to hear this comment if you have access to see from this page.
Am came from Chikwawa district and kuzombakuno its just school.
People may talk slot about you but please stand as per what God has called you to be in life. We wish you all the best as you forward move forward not in talent but in your calling. Embrace this opportunity that God has trusted you with.
all the best join Evangelism as your husband is doing there is souls that need salvation and your called for holiness not uncleaneness.
ok
Timvera
Mulli. Wakuthawa watha napulani