Very good article. Lazarus is a delusioned person. He still thinks he is a president and not Peter. Lets wait when he wakes up from his dreams probably in 2020
sekunda
9 years ago
Kasi muli a chizende? Kulemba konse uko ndiganiza mulemba volongosoka. Muzikhara nanzeru wawa.
Modern Malawi
9 years ago
Abusa mutu wawo sukugwira bwino bwino chithawireni ntchito ya u busa,pepani a busa akale
zikuoneka kuti mpando umenewu simuzakhalapo,mukukumbukira pa 17 May munagundika kupemphera mutakweza manja kaya mmathokoza kaya ku pempha Mulungu? Munaoneka pa front page ya nyuzi pepala ngati zeni zeni, Munaona
bwanji zomwe Mulungu anakupangani? Mulumgu simungapange nawo zamasanje ayi,kulibwino ku bwelera ku mpingo basi.
Kkkkk anthu akagona amalota ali m,boma ndiye apange bwanji? Anathawa ntchito ya ambuye kufuna u commander in-chief ndiye kuti 10 years ithe ndiliti? Kungokhala shadow yemweyo kkkk nanenso shadow speaker of parliament kkkk
Checheche Munthali
9 years ago
MY BROTHER GEDION, I THINK YOU HAVE MISSED A POINT. SAMALA YOUR CAREER FIRST BEFORE EATING IDIOT’S MONEY. MWANAWAKWITHU WACHITA VICHI……GEDION GEDION BWANJI……………….
Very good article. Lazarus is a delusioned person. He still thinks he is a president and not Peter. Lets wait when he wakes up from his dreams probably in 2020
Kasi muli a chizende? Kulemba konse uko ndiganiza mulemba volongosoka. Muzikhara nanzeru wawa.
Abusa mutu wawo sukugwira bwino bwino chithawireni ntchito ya u busa,pepani a busa akale
zikuoneka kuti mpando umenewu simuzakhalapo,mukukumbukira pa 17 May munagundika kupemphera mutakweza manja kaya mmathokoza kaya ku pempha Mulungu? Munaoneka pa front page ya nyuzi pepala ngati zeni zeni, Munaona
bwanji zomwe Mulungu anakupangani? Mulumgu simungapange nawo zamasanje ayi,kulibwino ku bwelera ku mpingo basi.
mukufuna kutchuka kuti mmatha kulemba eti? IWE WALEMBAWE UDZAFA IMFA YOWAWA.
Kodi mumangolembapo zinthu poti mmanja mwanumo mwagwira cholembera, kapena mumayamba kaye mwaginiza bwinobwino nkuchita kafukufuku? Why do you choose to live behind civilization? Inu simukuona kuti Chakwera akupanga ndale zoenerera in a democratic society? Ndakumvetsani, paja enanu munazolowera ndale zonyenyana-nyenyana.
I think having a shadow cabinet shows how responsible the MCP is.
SAMALANI TCHITO YINU SIBWENI,WAMUTUMANI MUFWENGE NYIFWA YAKUWAWA PALA MWALUTILIZGA.
Kikikiki useless article
Kkkkk anthu akagona amalota ali m,boma ndiye apange bwanji? Anathawa ntchito ya ambuye kufuna u commander in-chief ndiye kuti 10 years ithe ndiliti? Kungokhala shadow yemweyo kkkk nanenso shadow speaker of parliament kkkk
MY BROTHER GEDION, I THINK YOU HAVE MISSED A POINT. SAMALA YOUR CAREER FIRST BEFORE EATING IDIOT’S MONEY. MWANAWAKWITHU WACHITA VICHI……GEDION GEDION BWANJI……………….