Fire guts Kasungu market
Malawians are now used to fire gutting markets. It has become the order of the day and the latest market to go up in Flames is Kasungu in the central region tobacco growing district.
Property worth millions of Kwacha at Kasungu market has been destroyed as fire reduced the shops to mere smouldering rubble.
The cause of the fire is yet to be established.
The incident follows another recently where Lilongwe Area 18 market, Tsoka Flea Market and Mzuzu market were also destroyed.
President Peter Peter Mutharika instituted a ministerial committee to look into the occurrences and come up with lasting solutions to the problem.
Koma zinazi, ngati tikumachitira dala kuotcha misika mwadala ncholinga chofuna kuti boma litithandizepo tiyambe tawona kuti boma lathu lili ndi vuto la ndalama komanso lili ndi zochita zina ndi ndalama. Akazalekerera tidzaona ngati sakutifuna. It is so smpathetic to be hearing the same now and again. Ngozi zina zingathe kupewedwa ndipo opewa ndi eni ake amalowo (a ma business). Nditengereponso mwayi monga ngati kukokoloka kwa anzathu ku Chikhwawa, Mangochi mu nthawi ya mvulayi, Boma lidayamba kalekale kuwauza kuti mmadera amenewo asamukeko akakhale kumalo abwino ndipo panali nkhani yakuzigulira malo. Koma we need to see the consequence before we take the… Read more »
Fire guts kasungu market but mr our president r nt atend that accedent so mi fell malawian z it malawi there z agood leader,if we r agud leader xo y r nt atend of dc acc
Amalawi tichitepo kanthu pampnkha ya msika wa abale athu ku kasungu,
HOW DOES THE FIRE CONCERN PRESIDENT CHAKWERA???….IZI SIZANDALE OUR FRIENDS ARE IN SERIOUS TROUBLE….THE SOURCE OF THEIR LIVELIHOOD IS GONE…NGATI TILIBE CHONENA CHANZERU BWANJI TIZINGOKHALA A MALAWI ANZANGA!!!!!!!!!!!!!!!!
after all the finger pointing what do we have for those affected. I don’t think our arguments are helping. my opinion is town assemblies should learn something ppl build shops shops with what ever cheap planks and boards they can find and to me these will just escalate fire in case of such accidents. aren’t markets supposed to be devpd according to plans?. who is responsible to ensure safety of goods of these hard working Malawians in kasungu?. take the town councils to court please for they have breached their duty of care. u deserve remedies in damages to the… Read more »
Iwe #1 comment, Tatya nose like musca domestica, your head is full of maggots.. Machende ako mwana wa hule.
God knws the truth of the matter,,,,,
Perhaps h wll judge by hmslf
hu starts da fire in da dfrnt markets
Chakwera the fireman of Nyau Party is the one behind all this. Machesi ali thoo mmanja. This pastor of yours simply wants to make campaign at burnt markets one after another. Next time mr fireman chakwera will burn his very podium.
Shame on you MCP president! How can you stoop so low setting markets on fire only to rush there as a sympathiser. This is hypocrisy of the highest order, stop this madness bwana Chakwera.
Nthawi ya Bakali boma linatumiza anthu Ku Zambia kuti akaone mmene anamangira City Market kuti kuno amange chimodzi modzi koma nkhani yake sinaoneke kumene Inathera anthu akuti mwa wayika kutali ndi Bus Depot. Misika kungokhala ngati zopangiramo zawana. Pamphaninso a China amange misika yabwino anthu amalipira City rent. Tsono mutani nao Nanga pakuti alive ndalama. Naonso anthu ndiye anangoziwa umphawi . Ka malo komwe akulentako kukadula pangapo ati nao kulentetsa Iwo za lenti zisamatuluke. Ndi katundu kugoti thithi ngati chani kaya ati kutengera Ku kiyera. Poti kumanga msika sichithu chofumika nsanga pakali Pano poti pali vuto la chakudya ndi chipatala… Read more »