Email a copy of 'First Lady’s aide booted out of State House' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'First Lady’s aide booted out of State House' to a friend
It was a day of emotions and unity of purpose for Malawi as dignitaries, politicians and people from all walks...
God save Malawi from bad behaviours
Ntchafu kapena kantchafu? Shupiti woman, kuonekanso kuti makomedwe mulibemo.
Please chonde azimai dzisamalirani kuvala nanga mpaka chonchi tchafu?
THIS IS WHAT I SAID PREVIUOSLY, STILL THE GAME IS NOT OVER, WAIT MORE ARE IN THE RING AND OTHER SEALED BOXES ARE NOT OPENED YET. MORE FIRE ON THE WAY.
Amina , muwonesese bwino fotoi ! Mai wa zawhite wakhala pampando , manja ,manja wakoleka pa mpando . Sinchafu ai. Onesesani bwino bwino
NO 41, imeneyo ndi ntchafu. Kodi ndani akudziwa mwiniwake wa ntchafuyo? mwaiona bwanji?
away from the story is the person sitting next to the first lady wearing anything below her buttocks? Pliz whoever has good eyes let me know. Akukhala ngati sanavale chili chonsetu. kikiki! Kunali kuti kumeneko?
Chitukuko pa Malawi, ntcha izo m’boma, imeneyo si Cash Gate iyayi ndi Cash Man!
tyme-tyme
Uthenga wanga kwa President wadziko Lino ndi inu nonse andale. Would you please leave the professional jobs to professionals and let politicians do their politics. It is demoralizing to professionals. Zoona ma cadet azikhala akulamulira munthu woti akuiziwa ntchito do you expect kuti zinthu zingayende? Ngati dziko Lino lisakitukuka nkhani Ina ikuvuta ndi imeneyi. Mukumatenga ma cadet kumawapasa maudindo mma institutions aboma cholinga azibamo. Bwanji simumakawasiya ku defense force or police mumaopa chani. Ndichimozimozi ndi MRA sangazikwanise zinthuzi ziwauikani malo oyenera