Email a copy of 'First Merchant Bank robbery prime suspect Malunga dies' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'First Merchant Bank robbery prime suspect Malunga dies' to a friend
Premier mobile service provider TNM today proudly announces the donation ofK6 million to Malawi Blood Transfusion Service (MBTS) to help...
ku TZ akagwira mbava kwake kwatha thus umbava ndiochepa kwa anzathu. ku malawi apolisi kumwa bawa ndi mbava kenako hire mfuti kuti mbavazo zikabere. mulungu ngwamayankhi adzayankha
Big up police anthu amenewa afebasi
Mbava zoipa ndi a policewa amalawi,mfuti amatenga ndiwo kupangitsa hire kwa mbavazi,boma lionetsetse genesis wa umbava nchifukwa amwapanga bail mwachangu,Pelekani mesa ankangoyenda thimalirizii;”akazi anga ndi bwana ku BLATYRE POLICE”,banja linatherakuti? Mwapereka umboni? Mulunguwathu salolnso kuti munjoye ife misozi ilimbwembwembwe m’maso,MALAWI UNALI WABWINO KAMUZU ALIPO IWE!!
eya ntchito ilipo ku jehenako, mukaona kuti Jesus ndi dolo RIP
They should not die before revealing their friends and bosses. Why are they dying before taken to court? A Polisi pano ndiye mwawonjeza. We are suffering yet the real robbers are these men in uniform. You steal from the roads during the day and with guns during the night.
We would have loved to see his photo…
utenge ndi futi yako yomweyo aise pelekani malunga uzikabera kupaladaizo.
Anthuni musathamangile kusekelera kuti Malunga wafa. Kodi tinawuzidwa ngati ndalama anabazo zinayendesedwa bwanji. Malunga atamangidwa anawulala chiyai? Nkhaniyi ili ndi zibowo zambiri.
Perekani wapereka moyo wake mopusa… Umati chani pwanga each dog has its day. Six feet pwanga akumangirenso concrete kenako chipilala uziba kumanda komweko galu. Koma ndibwera kumaliro ako osadanda pwanga
Chilichonse chouluka tsiku lina chidzatera….