Email a copy of 'Five killed in Mzuzu road fatality, dozens seriously injured' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Five killed in Mzuzu road fatality, dozens seriously injured' to a friend
United Democratic Front (UDF) president Atupele Muluzi has said he is ready to put his party on an election footing but...
Bus Depots should also have authorities who can enforce loading capacity. For example at Lilongwe main Bus Depot there is a police office but buses leave overloaded (what is their duty there, kugwira mavenda basi?) and you expect the bus to be checked somewhere after it has already left. A Malawi lets also use the free toll number 4040 to alert the Road Traffic Directorate of any traffic violations.
Aboma mutithandize chifukwa malamulo mumaikawa sagwira ntchito ndipo amaononga malamulo ndikuphetsa anthu mumisewumu ndi a polisi anu a traffif. Iwo amakhala busy ndi ziphuphu kumadutsitsa ma bus/minibus a overloaded ndi kandalama kochepa kamene amalandira kuchokera kwa ma conductor. Zimatimvetsa chisoni kuona mmene amalandilira ndalamazo. Ndiye poti osauka alibe mau basi tizingofa ngati nkhuku zachitopa choncho. Koma pano tizitenga ma video chifukwa tayamba kuyera mmaso pano ndipo auzeni ma traffic officerwo kuti achenjere polandira ndalamazi pano. Koma a President chitanipo kanthu ku traffic office. Munthu sungakhoze mayeso a traffic pano kuti akupatse licence without ndalama pano ayi. Ntaonankoni uku a president… Read more »
Bus are always overloaded. What’s more disappointing is that the police at road blocks such as Dunduzu and Lusangazi are sleeping on the job. Instead of enforcing traffic rules (e.g.) checking capacity of buses they are busy taking bribes.
Can government issue a directive that from now on, no bus will be overloaded? Any overloaded bus will be impounded. The same applies to mini buses. Govt must be serious.