Email a copy of 'From 'Ziphwisi' law, trust Malawi Minister Chaponda to say ridiculous things' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

45 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Alungwana
Alungwana
8 years ago

As citizens of Malawi, we are supposed to know how our taxes are being spent. It is therefore unfair for George Chaponda to tell the journalist that he was wasting time.

Makhuwira
Makhuwira
8 years ago

Dr Chaponda amaoneka ngati sa samba kapena ku samba mankhwala

Kashot bernat
Kashot bernat
8 years ago

Don’t worry malawians God sees beyond the sea angatizuze bwanji koma one day is one day adzazisiya basi ngati m`bale wake uja

Thako la njoka
Thako la njoka
8 years ago

He realy fatted here,had he known how tough life of a malawian thobwa seller is,he wouldnt spoke it.
Mbuzi za anthu mukafika 2019 muli ndi mwayi.

Mfumu yachewa kumphoto
Mfumu yachewa kumphoto
8 years ago

Koseko ndkulephera

Dr Chaponda
8 years ago

Musadandaule achimwene, ineyo ndamene ndalakwitsa, zonse adziwa n’mulungu. Munditumizire account number yanu, ndugawireniko kangachepe.

Douglas Ndindi
Douglas Ndindi
8 years ago

Enanu mwati dzana lanu ndinu a Matako a Pusi? Ndiye mwati tidzipatsana ulemu? Lanulo ndi dzana la munthu woti angalangize anthu kuti tidzipatsana ulemu? Ingokhalani chete.

Dr Chaponda
8 years ago

Zonse zomwe mwanena ndamva, vuto si ine ayi koma nkhope yangayi.

Dr Chaponda
8 years ago
Reply to  Dr Chaponda

Muzingovutika ine ndikudya ndalama zanu m’bomamu. Kukhala minister simaseweratu, kuteroko umphawi ndi omwe ukukubwebwetetsani. Ine ndiye wakubayo. Kodi nkhope yangayi siimakuopsani? Dikirani kaye, ndimayenda nditatsinzinatu ine?

che Mbela
che Mbela
8 years ago

Dziko lotembeleredwa lino. Kumangosankha atsogoleri opanda chidwi ndi mabvuto a dziko lomwe akulamula.

phiri Gabriel
8 years ago

Truly, the minister should appreciate that playing the smart card guy will not bring back donors.

Read previous post:
Kwacha! Kandodo returns to Malawi Congress Party -Report

Malawi Congress Party (MCP) continue to gain more ground and attract more members with the latest being former cabinet minister...

Close