Email a copy of 'Germany gives Malawi K48bn development aid: Impressed with fight against corruption' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

33 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
sendela
sendela
5 years ago

boma its a big place where opportunity are found osati basi azingodyelela achina dausi , henry mussa , mchacha, mr maliseche antuwoso osayamika kubaso ndalama , achokemo mboma ameneo kubwele antu ena aone mumene moyo umawawila ukakala kunja kwa boma kuzolowela za ulele

Petersburg
Petersburg
5 years ago

a dpp simungakwezeso bar kuposa pamenepa , mwatopa mwakulaso, ma development amene mukuwanena a ma cadet mumaona inuyo noka enafe timsngoona cashgate 145 million , in someone pockets yemwe ndiwosayamika chifukwa amalawi anamupasa ulemelelo povota 2014 kulemela pompompo pambuyo wamela mizu wayamba kuona ngati ndalama zonse aziziba, ndi apumbwa nothing more can offer the best for them now is to retire ndipo amalawi tiyesese akupumedi pa 21/may/2019 anyamata angono angono asamakale opanda nchito wina Wa zaka 80 alimu office , Malawians wake up let’s give the opportunity to the youth nditawi yawo nawoso are educate like them komaso more energetic… Read more »

Apumbwa
Apumbwa
5 years ago

Another CASHGATE in the making thank you Germany!!!

Kanyimbi
Kanyimbi
5 years ago

Apumbwa a DPP mukuyesa Germany ndiyopusa ndalamazo zidzera ku GIZ ndimabungwe ena a ku Germany omwe amatumikira m’Malawi muno sidzipita ku treasury kwa Goodall Pumbwa Gondwe, chizungu chake akuti The Grant Will Be Channelled Through Germany Agencies. Germany ndi ulemu chabe ponena kuti DPP ikulimbana ndi katangale aaaah! zoona mukubvomera zimenezi ana a dad kuti APM anamangapo munthu kupita ku ndende coz of kuba?

concerned citizen
concerned citizen
5 years ago

Operekawo mwina sanamve za 54billion yomwe yasowetsedwa kweninkweniko ku OPC.

Kibaki
Kibaki
5 years ago

Which Corruption? amayooòoo ine. The whole world is corrupt.

mtete
mtete
5 years ago

The West is very uncomfortable with the inroads China is making in Africa generally and Malawi in particular to the extent countries like Germany will assist even plunderers of public resources. What efforts in fighting corruption are these Germans talking about when it’s so plain and clear even the president is a beneficiary of stolen money? Remember K145m?

braveheart
5 years ago

Salute!

Shack
Shack
5 years ago

Which fight against corruption? The Office of the President is leading in swindling taxpayers money according to the report that came out yesterday. K54 billion swindled and OPC is in the lead.

phakamani mahlambi
5 years ago

chi big pumbwa kusekelela kwambiri kuti chidyenso money ngaati mmene chimachitila ndi ma 145 mita aja!!!!!!!!!

Read previous post:
Lacha replaces Usi as ADRA Malawi top boss: Mhango new Programs Director

Adventist Development and Relief Agency (ADRA) Malawi has a new Acting Chief Executive Officer in the name of Hastings Jabulani...

Close