Email a copy of 'Growing calls for Lilongwe Mayor Bikoko to resign ' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

19 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
SKC
SKC
5 years ago

Tikamuotcha Bikoko enawa atengerapo mphunzilo, Bikoko tichete chowotcha ndukuuzani a Malawi mbava zinzake sizizayiwala sizakhala ndi mantha moyo wake onse, Bikoko tiotche basi ndipatseni address yake chonde. Muno mu Lilongwe za chamba ayi Bikoko atenthedwe basi chifukwa akapita ku court Munthalika akamutulutsa kuti osalakwa, ngati anakwanitsa kuotcha Njaunju osalakwa tilephera bwanji kuotchaBikoko, address ya Bikoko ndichiyani I mean physical address ya Bikoko, maloakugulitsa ana tikuberekawa azakakhala kuti, amwenye ma Burundi, Nigeria Mozambique akugula malomwa chinyengo kwabasi, Bikoko Bikoko samala mayendedwe ako

mapuyamurupare
mapuyamurupare
5 years ago

Ku Thyolo chief Executive achoke chifukwa chosamvela malangizo a makhansala komanso akuluakulu a business ndi Mafumu. Ndalama za nkhani – nkhani Zasakazika pomanga council rest house pamalo pamene pakumangidwanso stadium ndipo rest house yatsopa yagumulidwa, office yomangidwa kale ya anyamata ndi atsikana ya TAYO anagumula. Chitukuko palibe chikupita mmbuyo.. Chifukwa chosamvela malangizo Ana asukulu a kusowa bwalo losewelapo mpila chifukwa stadium yomangidwa paground lakale ngati muthyolo malo anatha pofuna kuwalemekeza amwenye amene agula malo athu ama estate. HIV ya koleranso pakati pa achinyamata chifuka chotsowa malo omenyera mpira. Stadium yanyuwani ikamatha anyamatanso atatha not AIDS. Executive Officer kulephera kukapempha malo… Read more »

Ntengo wa Kesia
Ntengo wa Kesia
5 years ago

Bikoko achoke yekha … otherwise ma demo basi. Ma CSO tiuseni, ndipo tiuzeni tipanga liti ma demowo?
Pofunika tiike Mchewa weni weni pampando umenewu.
Tisamalole mitundu ina. Asa.

SKC
SKC
5 years ago

Start the discussion…Bikoko yu akagwidwa kungomuotcha basi ndiwausile, abale tandipatsani address ya komwe amakhala.

kaka ni dada
kaka ni dada
5 years ago

I wonder why thieves associate themselves with DPP. Dumping MCP to join DPP in order to steal from Malawians. Shame on Bikoko.

Achiswe
5 years ago

‘Our mayor is now a porn in the game of thieves.’ This should read; ‘Our mayor is now a pawn in the game of thieves’. The word ‘pawn’ is a reference to a piece in the game of chess which is often sacrificed to gain an advantage. Unfortunately words are frequently misused on this website. People have heard a word used but then misspell it due to confusing it with another word that sounds the same or almost the same.

ndele
ndele
5 years ago

cimutu congodzaza ndi mafinya ichi. ma bastard awa ongokonda ndalama ndi azimai. full of buullshit asshole.
ife tikumavuta kaamba ka anthu ngati inu. tisankhe ophuzila anta ,tisankhe osaphuzila anta. nde tilowere kuti AMBUYE TIPULUMUSENI KWA MIN;GAZI YOKUBA IYI

Kaitano
Kaitano
5 years ago

I think we Malawians are to blame, by just looking at this Bikoko landgate, it has just proved that seriously we have a side and or a room where people meet and have a very good time to discuss how to eat our sweat, this guy was once in MCP he saw that the leadership in that Party can not tolerate what he wanted, that is why he left and joining the team which knows where the room is and what time they met and what do they do, Malawians sometimes we need to know that we may chose not… Read more »

DAVIE C MAKAWA
5 years ago

bikoko you left MCP because you knew by joining DPP you will have immunity against any corrupt practices you may be involved in, now you want the people to suffer your corruption? whatch out my dear.

Yahya Yahya Jammeh
5 years ago

Someone with a PhD and you opt to join politics, does that suggest that you have been successful with your PhD and a PhD in what? By the way what was Bikoko doing with his PhD before he came into the fore? Perhaps, his past record would give us a rough picture about him for proper diagnosis of his character and ability. It is slowly becoming apparent these days that people with PhDs and are under-performing are drifting to politics because it is the easiest career one can follow if they are good at telling lies.

Read previous post:
RVG facilitates Belgium trials for two Malawi players: Precious Sambani and Peter Banda

Two Malawian players are expected to undergo trials at a Belgian League Champions club Brugge thanks to Flames Coach Roy...

Close