Email a copy of 'Gwaladi out on bail: Malawi singer faces sex assault rap' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

42 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
amfana
8 years ago

Mwanayu ndichibwenzi chake kungoti tsikulo sadamupase dola.mutayeni akakwerenso wadzaka 10.

nazimbiri
nazimbiri
8 years ago

isaaa!uchitsiru kumachita kuyaluka nawo choncho,ngati ndinu nokha anatokupatsani nthumbwana(maliseche) mkabudura ogonera ana aanthu,katofota kameneko mukayamba kudwala,simumatopita ku kch mukaone anzanu momwe atovutitsira achibale ndi matenda amgonagona.imfa ya munthu ochimwa Mulungu samatosangalala nayo.alomwee alomweeeeee!mapwiya makaka

Said
8 years ago

Kodi nkaziyo amakataniko kuchipinda cha gwaladi. Khaniyo kumayiona bwino akuluakulu pls. Zogwilizana basi. Tangomuchajani gwaladi akapitilize luso lake loyimba kkkkkkk ati gwaladi ndiokongola dziko lose kkkkkkk uziona wakula watha. Cape town

Sulaimana amali
Sulaimana amali
8 years ago

Anyway tiona mmene zitathere

TEMACO INVESTMENT
TEMACO INVESTMENT
8 years ago

Koma anzathu a chewa mpaka akazi atatu munthu adakali mnyamata? Bola ife atumbuka tikumalera.

FELIX AP BANDA
FELIX AP BANDA
8 years ago

AYII ABALE AMAPANGA CHOOCHO?MAUDI AMALENGA MAN.LEROTU NDIIZOO WAZIMENYA DABOOKIKI.

Tchinga Chisoni
Tchinga Chisoni
8 years ago

Akuimbilani nyimbo muona

Pajogama
Pajogama
8 years ago

May God be with Gwaladi.

Chemtukanika
Chemtukanika
8 years ago

‘Ndikanadziwa sindikanapanga ee!Ndikanadziwa ndikuti sindikanachita ee!Lero ndagona mchitolokosi inee!Ena akuti ndi bodza,ena akuti ndi zoona!A khoti ndiwo adzagamule yee!………

Olobodoka
Olobodoka
8 years ago

Amkulu amalangizo wa asaaaa zimati iwo kupeleka malangizo abwino awa ntchito zapakamwa pawo zawachitira umboni ndikanadziwe eeeee sindikanapanga aaaaa nyimbo yake imeneyo kikikikikikikikiki……..

Read previous post:
Malawi assures American investors on security

President Professor Peter Mutharika Thursday assured American investors that the country will provide security to their business. Speaking at Kamuzu...

Close