Email a copy of 'Heavy rains, floods cause havoc in Mchinji: Maize gardens affected' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

4 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Chambe
Chambe
7 years ago

Chimanga cha mdimba ichi. Mvula yavumbayi ndi yobzalira chimanga kumene.
Nawo awa mukuti a Gumba awatu ndiye ai ndithu. Munthu opanda chitukuko kwa Mlonyeni ndi uyo. Mvulayi imagwa ali ku Lilongwe komwe amakhala. Izi ndizochita kumva osati zoona nthawi yomweyo.

Harawara
Harawara
7 years ago

Ohoooo my people!

wawa
wawa
7 years ago

@ Zoona zake! kukanakhala ku south bwezi Boma litatumiza kaye ma truck a relief items koma poti ndipakati …….ukuti bwanji?

Zoona zake
Zoona zake
7 years ago

Kukanakhala ku South bwenzi mukuti Mulungu wakwiya chifukwa chobera zisankho ndiye apa titi chani Tsano? Ooooh ndiye kuti chisankho MCP yawina posachedwapa chija inabera ndiye Mulungu wakwiya eti? Ndithandizeni amnzanga amene mumayankhula za mtunzu inu!

Read previous post:
Minister Chaponda behaves like ‘rattlesnake’, taunts MP Harry Mkandawire: Malawi Parliament

Minister of Agriculture, Irrigation and Water Development George Chaponda was subject to taunts and slurs in Parliament by Mzimba West MP,...

Close