Email a copy of 'I’m not a Satanist, Skeffa: Malawi musician hits at claims he worships the devil' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'I’m not a Satanist, Skeffa: Malawi musician hits at claims he worships the devil' to a friend
We are a God fearing nation-that is a fact, depending on which side of any debate you are. We have...
Mmmm guys yakula apa ndi sanje vuto lakwanthu kuno ndilimeneli moyo wachitsamunda osafunilana zabwino ngati zakuvutani osaipitsa anzanu pamene zawo zikutheka…
Mukamaipitsa mbiri ya anzanu muzikumbukira kuti Mulungu akuona ndipo akumva zokamba zanuzo,, kambani m’mene mungathele koma ife Skeffa timamukonda ndipo tizamukondabe
He’s stupid man. Dzina la ambuye basi lobixaliramo? Look @ him
Ndimamukondabe basi
ine sondupangs nawo ahahahahaa s usova
osalimbana amalawi chiweluzo ndi cha mulungu ekhabasi that is last day’s zoona angazidziwe ndi mulungu
Ufiti ulipo ndipo satana alipo bible says tsoka mtunda ndi nyanja popeza oyipayo watsikira komweko bt only God knows akanakhala kuti satana kulibe sibwenzi anthu akuvutika komasoi akufa komaso kuchimwa coz mtchimo linabwera ndi satana only Gknwa the truth abt skefa
Nthawi zambiri utsi sufuka popanda moto and thats the fact. Sangavomereze munthu oti akuchita choipa komanso chochititsa manyazi ngati chimenechi. Koamano chilungamo ndi choti “Actions shall be judged by their intention and every person shall be judged accordingly.
i love your music
Malawi wil neva dvelop due 2 jelousy