Email a copy of 'Injured Mangochi woman accuses DPP of neglecting her' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Injured Mangochi woman accuses DPP of neglecting her' to a friend
Malawi Congress Party (MCP) president and leader of opposition in Parliament Lazarus Chakwera has endorsed plans by the civil society...
Anthu timanyamulawo amadziwa kuti tiwapatsa K100 why complain sit in as a than size? Ife DPP timangofunako mavote anu. Bola anthu akwathu ku Mulanje nd Thyolo akutipanga support. Timawapasa zambiri ndipo kulibe wovutika kwathu. Onse akunjoya DPP.
MCP let’s go and see the lady. A little amount will help her. How I wish I was there to visit her on behalf of mcp.
This is an opportunity.
Aaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaa kuteleku mukumapatsana ma K100?
Kususuka azimai, mbava izi zikupweteketsaniiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii
A DPP chonde thandizani mai uyu Ali muchipatala ngakhare kumu uza APM akhoza kumuthandiza mai uyo.
Kutengeka azimayi!
that is how DPP supporters will be dumped after Elections.
Move away from dpp this is not the party for the heart of Malawians no come to Malawi Congress Party your destiny is live
my name is PATUMA TWAIBU kamba ndine nkazi ndikanakhala mamuna ndikanakhala che BATUMEYO TWAIBU KIKIKIKIKIKIKI FAKA MA NYEMBE, KUTSEKA KUTI HEEEEEEEE MIKANDA KUTI LAKATAAAA.
Kkkkkkkkkkkk midyomba, wakwiya ndi mfiti hahahahaha
KUMAONA CHIPANI CHOKACHIVINIRA……….ZOONA KUMAKAVINIRA CHIPANI CHAMAGAZI CHA DPP…..NDIZIMENEZOTU
DPP leaders, please hear her cry, what can k100 buy these days? You ferry people from distant areas to decorate your rallies but when a problem like this one arises you’re nowhere to be seen—mukugwa 2019 mwafa inu basi
Ulesi kukonda za ulere azikupatsani 100.00 yomweyo its enough. Mukufuna kulandira ndalama yoposa apa muli pantchito inu? Nonsense akamati zipitani ku sukulu mumatoyesa ngati apongozi. Phunzirani achina Che Biliati ndi achina abiti Patuma kkkkkkkkk