Email a copy of 'IPS enslaving Malawi tobacco farmers to poverty' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

5 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Terms and conditions apply

terms and conditions apply

patrick
patrick
8 years ago

Tobacco companies are looting Malawi, they are hoarding the forex couretsy of Reserve bank ruling allowing last year then to keep 100% of there export proceeds. This tobacco is for the farmers of malawi they pay peanuts to farmers and sell at high price around usd6 per kg and then they dont change the dollars they send them to there countries. This tobacco company should change there dollars immediately then kwacha can stabilise chifukwa ndalama za dollars akutumiza ku kwawo

Othana
Othana
8 years ago

Umbuli ndi matenda. IPS mwati ndi yoipa? loipa ndi Boma la Malawi. Why? Tobacco companies do not give farm inputs to farmers. The companies only stand as witnesses between farmers and banks. Commercial banks give loans to farmers through companies. On the seller sheet, have you seen a deduction going to any tobacco company? The Malawi government cannot ask banks to give farm inputs to the farmers. Banks operate on interests. Umbuli ndi matendadi. kafukufuku muzifunsanso athu ozindikirako. Alimi ambiri akhala mumugwirizanio ndi ma company a fodya kwazaka 8 ngati amawabera bwanji sakuchoka?….. Nduna, MPs Akulu akulu a mboma, TCC,… Read more »

Pansimpanthete
Pansimpanthete
8 years ago

Abolish IPS .Let farmers be producers and buyers be buyers. The price which they offer doesnt tally we are losing out natural resources .They are not giving back.They are taking our treasures to there home countries.Warning if they see that we have no capacity to produce tob they will leave us and go to other countries shame to matherland.

thakolagalu
8 years ago

Ndifuna ndivomerezane nawo alimi azanga amene adandaulawa. Ndizowona IPS inabwera kudzatisaukitsa ife alimi afodya, ndipo panopa tiri paukapolo zedi. Zimene akunena abwana aku TAMA ndi bodza la mkunkhuniza, chifukwa chimene chimachitka ndichoti ogula fodya amabweza kwambiri fodya wa ku chipandepande ndi cholinga chofuna kuumiriza mlimi kuti alowe pa contract. Inu mudamvapo kuti ngongole amachita chokakamiza? Ife olimi omatikakamiza kusaina(contract) ngongole zawozo, pozindikira kuti sititha kuwerengetsa bwino bwino. Pambuyo pake tindalama tonse tomwe m’limi amapeza pachaka timathera ngongole ndipo ngongoleyo imawolokera chaka chotsatira. Alimi amene adachitako mwayi mbuyomo, nagulako magalimoto kuti azinyamulira fodya wao amakakamizidwa kudzera ku timabungwe tosadziwika bwinobwino tomwe… Read more »

Read previous post:
Malawi PSs shuffled: Sande, Kang’ombe retire

Malawi government has shuffled principal secretaries (PSs) following the retirement of Commissioner for Disaster and PSs in the office of...

Close