Email a copy of 'Jesus stars at Nomads 4-0 humiliation in DR Congo: CAF Champions League' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

9 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Kinte
Kinte
6 years ago

Wanderers wammakwalala imautha koma CAF mwachepa muli kutali kwambiri

yazula
yazula
6 years ago

Neba! neba! neba! walira chokweza, komabe all in all mwina kuno ku mudzi udzalimba udzationetsa ma miracle goals Eeeeeish koma yaaa, AS Vita ndi akatundu omanga ndi mawaya guys mmmmm ine chonene ndilibe mpaka 4 goals kwa tetete?Where were you Malata,Sanudi,Nyirenda Hurry?KKKKKKKKKKKK!!!!!!!

CHIPYERELO
CHIPYERELO
6 years ago

I questioned the reasoning of joining CAF as I doubted the strength of the team. Wanderers failed to beat any of the top four teams last season in all competitions – CIVO, Bullets and Silver. They won the league by beating middle and bottom placed teams.

Kangoma
Kangoma
6 years ago

Koma ndiye kunali kuthamangitsidwa! eeeeeeeeeeeee Manyozo amvekere ziiii zibayo zokha zokha.

pathfinder
pathfinder
6 years ago

KKKKKKKK Tinkanena ife Nomads have no teeth. What an embarrassment?

Neba
Neba
6 years ago

Neba watichititsa manyazi ku dziko laeni. Unangopita kukavina kwasakwasa!!

Safari
Safari
6 years ago

Pepani neighbour ! ANTHU aku DRC alibe chisoni ndikubereka kwa anzawo. Kutizimula ana anzawo mosayangana nkhope. Pepani pepani malilo nkulilarana !!!

Awize
Awize
6 years ago
Reply to  Safari

Sad news for Nomads family. Train hard and become fit for men’s football. Best luck for your return leg match.

kwacha malawi
kwacha malawi
6 years ago
Reply to  Safari

Pitaninso mukawachangamirenso monga muja mudachitira muja powaperekeza. Izi ndi zaziii kuno ku Malawi tinacholowera mpira osewera pakamwa osati pa ground ai. Mpaka 4-0 a Madeira munali kuti ndi mzungu wanu uja Osman. Tinanena ife nkofunika kusintha Coach lero mwazioona kuno adzakuthirani 3-0 believe you me.

Read previous post:
Mutharika to partner Msaka as running mate

President Peter Mutharika has settled to pick Education Minister Bright Msaka as his running mate in the 2019 elections, Nyasa...

Close