Email a copy of 'Joyce Banda meets US Secretary of State John Kerry: Speaks to Harvard University students on women leadership' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Joyce Banda meets US Secretary of State John Kerry: Speaks to Harvard University students on women leadership' to a friend
After playing for several years without winning any silverware, Civo Service United Football Club have this time around vowed to...
More Fire Mama!
This is bullshit, what for????? at this state of affairs busy addressing women shit for what?????? Fuck that, fuck that US secretary fuck the students, fuck anybody who was there fuck you all
Omayi kuno kuli njala chaka chino kazibwerani mudzatiphikire nsima!!!!!!
Proper leadership and governance need wisdom and intelligence.
Amayi bwerani kumuzi.Bububu anatipatsa mbwiye Mbendera atalira ching’ang’adza angoba kuno, kulandira ziphuphu kwamwenye ndi ma lebanese ndinso kungosolola nkumatikalipira ngati ife timadya kunyumba kwache.Mbuzi ya mano kunsi-iyeyo amati Nyaphaphi!
NYAPHAPHI DZIKO LAKUKANIKA ILI
Mayi pamene zafikapa ndi Boma la dpp.li… Tazindikila kut ofunikila ndi inu.. Kuno zinthu zanyasa.. Bwelan amama… Muzatiphule kumotooooo
Amai tabwerani kuno mudzathetse milandu. u will not be persecuted but prosecuted. Asiyeni azunguwo kaya mukumana ndi ndani kaya ndani mudze kuno. Mantha ngati khwangwala baasi. unamumva mzungu uja, atitu big fish itofunika, motl
mmene u were shakn hands ndi azunguwo mumtima mwawo amangoti BIG FISH ija ndiimeneyi, kumakuaekelelaaa iwe uli mweeeeeee azungu azungu, akusewera ndi BIG FISH
Ena akapita kumeneko amakomana ndi ma councilors’ inu mpaka J K mpaka Ku Harvard University azungu amakukondani heavy koma manyasa samakukondani. Okondedwa ndi azungu ededwa ndi manyasa mwaona manje
Point taken,these whites have all machinary to know what is actually happening in other countries. They know that DPP is waste genesis and waste plunder of state resources in Malawi.They know that Joice Banda just inherited the system and continued it for her PP. They that know she has the right information about cashgate and started it being well linked with DPP. Donors will never have trust in DPP. Malawi will suffer under DPP and don’t cheat ourselves that Malawi survive well without western Doors.May be in 30 yrs time but for the time being its is a long way… Read more »
Malawians Lets Recommend What The Former State President Is Doing She Is Doing This To Influence Some Pple Who Can Assist This Collapsing Economy