Email a copy of 'Joyce Banda presents UN award to Girl Up Advocate: International Women’s Day' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Joyce Banda presents UN award to Girl Up Advocate: International Women’s Day' to a friend
The First Lady Gertrude Mutharika on Friday led women in the country in commemorating Womens World Day of Prayers with...
Nonse amene mukumuyikira kumbuyo za cashgate Joyce ndinu anthu oipa kwambiri munthuyu wawononga dzikoli. Atsogoleri onse amene anabanso mmbuyomu alingati Joyce yemweyi palibepo wabwino apa. Dziko la Malawi ndi lomvetsa chisoni kwambiri. Let the almighty fight for us and put the right people in power Amen.
Why despising Joyce Banda as if she is spending govt penny on her continued stay in USA? If you dpp fools have issues then bring them forward instead of wasting time attacking her for no apparent reason. Why are you interested in her coming back to malawi instead of feeling sorry on your president whose own ADC had an affair with Getu. Zamanyazi
Mama I love you! Keep up with the good job.
This woman is truly a disgrace, why not just come back home and clear her name in the courts? A whole fully grown former president running away from the mess that she created like a common thief? Shame!
Amalawi, kuzolowera kukweza changa mu mtengo
As usual, Malawians on this Forum are busy praising this politician and that. Instead of coming up with strategies to develop our households, communities and then our nation, people are busy glorifying politicians. Poor Malawi! No wonder we are a laughing stock. We will always keep on comparing regimes year in year out and staying stagnant in as far as development is concerned. Zonsezi coz we love receiving things instead of acquiring them through work, life of dependence. Zonse aakulemba the supporters of JB is coz asiya kudyerera. Nawonso enawo akuchita defend APM coz akudyetera. Those that work hard cannot… Read more »
Chendausiku ndiwe bakha! Makoyo anawina ndalama anabazo not elections. Akuthawa chani?kodi anthu akumamuitanawa sakudziwa mavuto anatisiyila nambava amaneu? utchisi eti asazabwelenso
Jb doing it
Akakhala atcheya akuti milandu yatha mai bwelani basi
Mayi wanu tilibe naye ntchito pa chichewa pali mau akuti bwalo ku siyilana musiyeni Peter avineko mayi zaka ziwiri alowa chifukwa chalamulo paleka uboni wabera mavoti kuganiza moperewera mawailesi amalengeza mofanana tiyeni tiyang’ane chitsongolo .