Email a copy of 'Joyce Banda to be quizzed on Malawi presidential jet ‘batter’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

12 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Charlie brown
Charlie brown
5 years ago

Nonse akuba ,Peter ,Joyce..you should also ask Joyce Banda about the torched escom building…Paja anawotcha ndi mwana wa mayi Joyce Banda..Thief’s everywhere

Zabura
Zabura
5 years ago

We fail to tackle cases and accomplish because everybody is corrupt but degree of corruption differs.Nkhani kuziyamba osawoneka komwe yathera. Kunali ya ndege chimanga zambiri kubgowononga ndalama pachabe.Amene sakufuna ya Ndege ndi ana amayi amadya nawo imeneyo ndi chimanga Brian Banda atha kuyankha bwino. K145 Million ndie amene sakufuna ipitilire ndi apanowa amene akudya nawo. CSO nthawi ya PP munkadya nawo palibe chitukuko ndi chimodzi chomwe amai anapanga koma kuva za ndege chimanga zida cash gate koma muli ziii phokoso simumapanga momwe mumachitira nthawi ya Bingu kapena lapanoli kodi kulira konseku mumafuna ndalamazi eti. CHANGE YOUR APPROACH BECAUSE YOU SEEM… Read more »

Zam'tonda
Zam'tonda
5 years ago

EedHey it is BARTER not batter change in spelling can simply peg whoever reads your reports in totally different world. Most of our Malawian journalists are illiterate they are lazy they don’t make an effort to go into the mind of the readers what impact an idle report has and remember that from good reports our children are good to learn about expansive writing. Bakili is dancing to corruption music in our courts the Malawi CSOs are baying for APMs resignation over Pioneer Investment sleaze the jet barter by our beloved JB is an additional dish to our corruption banquets.… Read more »

Nabanda
5 years ago

Zibwana zimenezi ai, chifukwa choti tikufuna mufotokozele bwinobwino mtundu wa a Malawi za MK145 million mukunama kuti ndi donation, ndiye mukubwelesa nkhani ya ndege? aaaaaah ai fotokozani ya fresh iyi. Palibe zozemba apa ai, APM ife a Malawi tikuvutika ndi umphawi, zoona mulibe chisoni muzingodya bwino nokha? I urge ACB to deal with the fresh story concerning the MK145 million, please!

Chilungamo
Chilungamo
5 years ago
Reply to  Nabanda

DPP knows most Malawians are a gullible lot & of coz easy to con. Especially the semi-illiterate poverty-stricken electorate from certain areas & regions the country.
Selfish & clueless DPP gurus pretty-well know will get away this such GRAND theft.
SHAME on MBAVA!!!

khodo
5 years ago

failed state ever seen in my life

Ujeni ujeni
Ujeni ujeni
5 years ago

Trying to divert the public attention to the K145m APM chopped

Ujeni ujeni
Ujeni ujeni
5 years ago

Trying to divert the K145m stolen money by APM

Sugzo
Sugzo
5 years ago

Why asknJoyce Banda as if she was directly responsible for the nitty gritty of the deal. I was in OPC that time if anything ask Ndilowe and Treasury.

Lupwito
Lupwito
5 years ago

Zayambika basi Amayi mphamvuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuu

Nalingula
Nalingula
5 years ago

kkkkk ati Titosiye kukamba za Pioneer tikambe za Amayi.Iri Nthawi ya Amayi bwenzi pano Pioneer ndi anzache ali Ku Chichiri.Ndi Amayi okha anamanga Anthu pa cashgate.Za 566billion kuli zii .Timangomva Bring me the Evidence …

Read previous post:
Ntata’s Uncommon Sense: Of Chilima’s parables and the quest for new politics in Malawi

Is the new way of doing politics that Vice President Saulos Chilima speaks about simply a matter of standing at...

Close