Email a copy of 'Joyce Banda to contest in 2019 polls: Analysts say Malawi's first female president chances of winning ‘very slim’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Joyce Banda to contest in 2019 polls: Analysts say Malawi's first female president chances of winning ‘very slim’' to a friend
The High Court in Blantyre is this Monday expected to start hearing Malawi's former president-for-life, Dr Hastings Kamuzu Banda property...
Amai, when you were assuming the care taker position Malawi had a presidential jet. When you left the country after losing the election Malawi had no presidential jet; kuononga kungapose apa. Anzanu omwe amanamizira farming Ku Mbalachanda with the assistance of your boy at Admarc are the ones who are keeping our jet. We want it since you are back bring it back as well.
MCP singawine chifukwa Chilima ndi wa pakati ndipo adzatapa mavoti a kongilesi. Mia ndi mkazache ndi akutsidwa. Kaliati anthu akwao amukana kale. DPP is intact. Kumbukilani 2014, kunali amai ndi cashgate yao, kunali Atupele koma DPP dribbled past them all. Chaka chino game ikhala yosavuta chifukwa Chakwera wagulitsa chipani Ku PP. Amene sakhulupilira angoona ndanda wa maina a NEC ya kongilesi apeza kuti akuluakulu onse achokera ku PP ndi eni ake a kongilesi ndi mamembala chabe mu komiti yaikuluyi. Angopakidwa mafuta a mbuzi pakamwa kuti anthu aziti adya nao uwende wa Sidik Mia. MCP ikugwanso 2019.
Simuzitha amayi.mudakanika with all the machinery and mumangokhalira kugawa ng’ombe. Mother and founder of cashgate. Convict Leonard Kalonga anakutchulani ku courts inu. Anywa zabwino zonse on 50:50 campaign. Mutithandize kugwetsa nkhalamba Pitala. Magetsi sankazimazima nthawi yanu.Pitala watsegulinso nsewo wanu.
Kkkkk all the comments i have read are just on the negative side onani nokha APA mayi kuti Malawians don’t want you again, kuthamanganso ndi mbuzi pa tala haha total madness nanga a agriculture azitani nanga aku social walfere
JOYCE BANDA,what else do you want? The billions of MK you stole and absconded was not enough,you want some more.What a greedy lady of Malawi? And why did you leave the country in secrecy and lived abroad for a number of years? This time you want to contest in the 2019 national elections,try on for the people of Malawi are still sleeping you might win.These people can even vote for H.Banda if he happens to come back from his grave!!! Joyce,what you did not accomplish when you were the President,you want to accomplish to-day? Joyce,do not take Malawians of today… Read more »
Amai, amai,amai zoona zimenezi?
Was it your son who arranged for escom to be torched ..She doesn’t deserve a second chance ,mai uyu kulalata
JB should in fact stand. The cashgate remains allegations. MBAVA sidzingapitilire the ones we have at the moment. They burn offices to eliminate evidence, connive to exonerate each other in court of law, FAKE official government letterheads, etc. If anything she is a lesser evil.
JB should not be discouraged, she may share the spoils with ‘tribal fiefdoms’ kind of voting in Malawi.
SHAME!!!
Thanks for the signal mama!! All the best!
Mbava yatulukira pati? Tiyionentsa.