Email a copy of 'Judge Kamwambe to rule on Muluzi case’s constitutional interpretation – Chief Jutsice' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Judge Kamwambe to rule on Muluzi case’s constitutional interpretation – Chief Jutsice' to a friend
Former students of Mangochi Secondary School (Masesco) in southern Malawi are planning anniversary celebrations marking 51 years of the schools...
God is the true Judge of everything, Bakili Muluzi still lives on today God had a reason for him to still be alive, yet the one who sentenced him Prof. Bingu died an embarrassing death. It doesn’t matter what the earthly judges like nyirenda have to say, God has the ultimate say in everything we do.. Time will tell!!!
ineyo sindifuna za kumachende zanditopetsa nyini zanu nonse ife anthu akumudzi tikuvutika coz of u pipo osowa chikondi ngati maluzi
Mwati zaka six mulandu umodzi?manyi anuo mukamapanga musamatiuze ife panopa tikuvutika kusowa chakudya ndiye olo mutiuze zamilandu zitipinduliranji?
Sindimaona chifukwa cholimbanilana ndi Muluzi ndalama zimenezo sikathu coz those days zinthu sizinali mmene zililimu anthu anali ndizonse zoyenera bola mulimbane ndi awa (cashgate staffs) amatenga mopanda chisoni pamene ziko likusowa ngakhale mankhwala amene eee nthawi ya a chair mukuti okubawo unalibe even makolo anthu akapita mzipatala amabwera ndi majumbo majumbo amakhwala, makope mmasukulu sinali nkhali nkhani taphunzisidwa ndi a chair ife even iwe ukuwelengawe. Let a chair be in peace
These guys are playing Poka on the people of Malawi ! one day some one bad will rise up and have them good !
CHILUNGAMO CHIKUSOWA NDITHU
MA BANK STATEMENT ONSEWO ALI MBWEE EEEEE !!!!
KOMA MUZITI IYAYI MULANDU WALOWA POLITICS ?,?
NKONA WANTHU TSOPANO TATOPA NAZO
TILUFUNA WOTATE WOCHAKWERA NDI ANZAWO
AZACHOTSE NYANSI ZIMENEZI BASI !!
Firstly we are fed up with this jargon of “Political persecution ” when politicians steals from the public coffers are being shielded by corrupt and immoral lawyers..The positions of the president has lifetime benefits for them and they think they have the right to steal from the Malawian citizen.We are fed up with these wrong winded cases that leads nowhere.No wonder Malawi is backward as ever because of shielding these thieving politicians.Why would somebody needs 60 cars at once?African politicians are very greedy while its subject are led into untold poverty.We need the truth about of 1.7 billion about thieving… Read more »
ndatha ine wanu Bwande, kuno ku malawi. koma mabvuto aku nyasaland azatha? musova kumalawiko ndikwacha wanuyo akungoyandama siku ndi siku.
Who knows who he does wrong before God? Surely ! Muluzi will never be charged anything on this isue before God because he was a good leader to everyone in malawi ,very flexible. I have never seen him before but God have recommended Muluzi to be a good leader forever more like David. Munthu uyu ndi wachikondi pa anthu ndipo zomwe amaononga pachikondi chomwe amachitira anthu zinali za ndalama za nkhanikhani koma samadandaula kalikonanse! Ndani akanatha kukonda anthu onse ngati Muluzi? Ndalama zokwana 1.7 b si kathu pamaso pa Mulungu. Zamziko ndizokutha izi osazitengera patali okay?
Zopanda ntchito izo tiyeni tiwasiye Atcheya apumule osawapingapinga ayi!!!