Email a copy of 'July 2011 demo victim families irked by Malawi govt delay to construct tombstones' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'July 2011 demo victim families irked by Malawi govt delay to construct tombstones' to a friend
Malawi’s Vice PresidentRight Honorable Saulos Chilima has called for increased student participation in sports saying sports and exercise in general...
Number # . .4 BATMAN whatever …# don’t think like headless chicken, this was DPP regime, Constitution law does not condone this inhuman conduct as this was unconstitutional, POLICE were instructed to monitor and police them not to kill citizens like mosquito belive you me even the THUGS, MURDERS and ROBBERIES you can name it all the way you wish…..????? but they deserved to be treated with dignity as they had RIGHT to LIFE no, no, no, no, no and no one can or may VIOLATE fundamental right. PLEASE do not JUDGE them ( victims) as they were protesting for… Read more »
A mayi ngati aluza ndi chifukwa chosaunikila choyenela kuyamba kuchitika pa chitukuko cha dziko. Nanga munthu ungalonjeze ziliza zipindula chani ku dziko pali zambili zofuna kuunikilidwa .No wonder she lost election and no tangible developmet during her 2 yr term.Her priority were upside down, Most of the victims were thugs , Nanga mwa anthu amene amatsogolela waphedwa ndani kusonyeza amayenda mu mseu . Okhao amene anasiya mseu kufuna kusautsa ena powabela ndi amene anakumana ndi tsoka lero mufuna akhale ma hero are we serious ngati dziko. Munsake JB amange boma ili ili ndi ntchito mankhwala apezeke mzipatala ,miseu ilimidwe ndi… Read more »
Aboma tangomangani zilizazo
Those pple were thugs not heroes dont mislead us
The government has no money to send to the grave. It is better if the money can be found to be sent to hospitals or prisons. by the way if the government has not built a tombstone on a grave of John Chilembwe who are these thieves to deserve our money?
No wonder this country cannot develop! Is this a priority for Malawi?
Mukuti amayi analonjeza kuti azamanga manda. Iwowo amalonjeza chifukwa nthawi imeneyo anali president. Tsopano poti upresident unapita kwa peter iwowo ayenela kupitiliza ntchito yomanga manda chifukwa nkhaniyi ndi ya boma. Maboma akamasintha nchitonso za boma zimapitilizidwa ndi ndi amene alowa mu boma. Apa tiwapemphe a boma ili la dpp kuti lithandize kumanga mandawa