Email a copy of 'Kalonga implicates Mphwiyo as Cashgate kingpin, testifies in Malawi High Court on looting crusade' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Kalonga implicates Mphwiyo as Cashgate kingpin, testifies in Malawi High Court on looting crusade' to a friend
Consumers Association of Malawi executive director, John Kapito, has blasted water utility body Lilongwe Water Board (LWB) following newspaper report...
@Chiling’oma, you sound so nervous…. why??? Calm down.
Kalonga is lying. He’s been influenced by DPP to cook up false allegations against PP and Amayi. Read the above story carefully. 1. Mr Makina, while travelling to the Airport, told Kalonga “he will link him to people that matter in government” to get diplomatic posts and realize his cherished dreams. Mr Makina immediately phoned someone who Kalonga alleges was Mphwiyo. When Kalonga meets “Mpwiyo” for the first time Mpwiyo also tells Kalonga “he will link him to people that matter in government”. Which people mattered in govt that both Makina and “Mpwiyo” referred to? When Makina talked about the… Read more »
Mphwiyo umbava kufuna kufelapo mpaka. Koma anthu munatasa inu. Koma kwatsala ma minister a DPP nao ayankhepo. Kuyambila anthu a ku diplomatic mission omwe anaba ma allowance a DRC a ma soldier nthawi yomwe anali ku UN Supuni ndi min of foreign affairs Chaponda pamodzi ndi Bowler. Zitangoululika munadziwa kuti UN ikumangani ur fellow mbava Peter removed you from UN foreign affairs to shield you..fokolo
On Mphwiyo evidence zero,guys milandu kumaitsata,am not backing him koma even Muli inuyo,munthu kukumana Mu Benz basi ukakhale Umboni??
Abale anzanga, Malawi is far gone on issues like this. Full of lies and thefts in the government, that’s why I don’t want to work in the government. Anthu okuba ndi a njiru ndi amene zawo akuti zikuwayendera bwino through mismanagement of government money. Ku MDF with the MDF Commander – Supuni being the No. 1 mbava. I still really don’t understand how Maulana was sucked as to me it shows the leadership is as well one of the top mbava as he is condoning liars and thieves. Wake up Malawi and bring back “Amayi” to answer what she knows… Read more »
Nkhani ndimeneyo, Akam lee po ndi MrCloud (Mr Mtambo from MHRC) muli kuti? Nanga muyankhulapo chiyani apa? kkkkkkkkk. Zagwera pa mphuno ya Kamlepo ndipo sazalankhulanso .Onse okubawa amangidwe ndipo ma key akatayidwe ku Lake Malombe.. I would love if all the so called CSOs to comment on the issue. Kaya poti nonse ndinu akuba simunenapo kanthu. Koma akanati ndi a boma eeshhhh.
Mphwiyo ukangotsogola ku ndende basi mkazi ndatenga. Tikwata ameneyo.
Bravo Kalonga wulula zonse. What about Makina poti it appears that his posting to the mission in Harare was a reward for stealing for Paul Mphwiyo, pamenepo Kalonga wulula Makina waba zingati kuti mpakana athandizidwe kupezeka akupita ku diplomatic posting ya PP. Tchwee mwana Tchweee PP woyeeee Oh Yes Amayi munakhazikika scheming ndi ma PS anu late Namathanga, Kandonje, late Njanji, Former Army Commander ndi Deputy wawo, Chisawawa of the highest order. Amayi muzabwelanso ku Malawi Kuno pokuti tsopano mulanduwu mufunika muzayikile umboni ha ha kkkk Cashgate woyeeeee
Ine pera magzu ghamala. Tunyatunya yese yura zikaba ndalama za unkhungu. PP watinyaza.
Tikazizwanga kuti makopala bakumwazika bakufuma kochi?
Kamlepo where are you? We need your comment here. So all this clandestine PP actions escaped Kamlepo’s wide eyes but could easily see Chaponda’s deals in Zambia? Koma kuli gule.