Email a copy of 'Kamlepo brands Chaponda ‘one of the most corrupt ministers’: No one prosecuted in K236bn Cashgate' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Kamlepo brands Chaponda ‘one of the most corrupt ministers’: No one prosecuted in K236bn Cashgate' to a friend
Member of Parliament for Lilongwe South (MCP) Peter Dimba has said Malawi is facing its worst crisis and that people are...
Chitsilu chikakhala chete anthu amachipna ngati chanzeru kpma chikalankhula chimaonetsa uchitsiru wake kunali bwino kamlepo akanakhala chete munthawi yake samanenepo sananenepo za Jb uladi lipenga mphwiyo kasambala msowoya ndi ena monga the then VP ambiri
More fire Kamlepo
This is malawi lets wait and see
TATULUTSANI REPORT
YAPA MUSAMANGOTOKOTA
WANTHU TIDZIWE ZANZENE
MUSAMANGOTIPUSITSA
MONGA A KASAMBALA
NDI ANZAWO A MPHWIYO
KUTI I WILL SPILL THE BEANS PAMENE AGWAMULA NDIWOWO. !
Sometimes even good messengers are seen as Devils not cause they are, but the beholders are…
Akuziwana! Tikuvutika ndiife anthu akumudzi.
We are tired of the stupidity of Kamlepo. Its long time people have been asking him to produce evidence of the 7 rotten ministers and give out their names. Akuluwa akukalamba ndi misala. And now the whole speaker is schooling Kamlepo and his communities that its their duty to produce evidence of any theft. Is this not embarrassing to him? We know that these guys are failures. They talked a lot in rallies about the 61bn of Bingu, later they talked of 92bn of Bingu’s administration. Despite being given 2 years to investigate their allegations they ended up arresting themselves.… Read more »
Pa central medical stores alipo so corruption wa ophya under buy malawi campaign from local manufacturers overcharging under the umbrella of being local manufacturers