Email a copy of 'Kananji ‘deserves to stay on’- Bullets' to a friend * Required Field Your Name: * Your E-Mail: * Your Remark: Friend's Name: * Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries. Friend's E-Mail: * Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries. Image Verification: * Loading ... Sharing is caring! 0 shares Share Tweet Pin LinkedIn Email Print
zimenezo nde ndizopuusa kwambiri. Konseku komwe wayikankha team yathuyi, kukonda ma foreigner bwanji instead of kutukulana
kungofuna kumutchukitsa munthu kut watengetsa leag pamene ntchito yonse wagwira ndi kananji musiyen m’ brund azipita holiday yatha asakomedwe kuno. Ine ndi wa nyerere
Kananji ali bwino kwa mbiri timusiye ayitenge team yathuyi osati mabodza enawo.
owo pangan manyiwo ife titenga mwala okanidwawo
kananji woyeee!!!
more fire kananji,,.
If BB succeed dis czon it’s simply bcoz of Elijah Kananji & not de so called Ramadhan! Pauzimba sizoloredwa ngakhale pang’ono kushomola nyama yomwe wapha mzako!!
Tiyeni tiupeze maullee!
KANANJI YEMWEYO ALI NYATWA GUYZ INU MUKUONA BWA???????????????????
Ine ndi wa nyerere koma palibe chifukwa chomveka kuti mungalembere ntchito mbulundi pamene team waipeza atakonza kale kananji kodi amalawi tinakhala bwanji nsanje? Ndikananji yemweyu akhoza kudzakocha frames mtsogolo simukudziwa? Kananji mpatseni ntchito nexst season osati ngatiso othandizira ayi
KANANJI YEMWEYO ALI BHOO