Email a copy of 'Karonga market shut down: Council force traders to pay revenue' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

21 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
apundi says
apundi says
9 years ago

musapereke ndalamazo ayi, zimapita kuti akachita makani a khonsolo memanani muotche ndi kuwagenda basi

Chimangenimapiko
Chimangenimapiko
9 years ago

An advice to all the market vendors in Malawi: Trading at council market is not a right. If you see that the market is not conducive to you, move on to a better market. You are not forced to trade in one market for life. Karonga council, use your by-laws to punish these stupid vendors. Close the market for a week adya matope amenewo.

kangaroo
kangaroo
9 years ago

Comment inu Atumbuka Lipilani rentals bwanji Kodi mtudzu?

Clement
Clement
9 years ago

Akukana kupeleka revenue wa ndiaku tanzania,matayifa sia malawi.ndiye kungowawuza kuti anyamuke basi

chidumayo
chidumayo
9 years ago

A Khonsolo kuba mavenda amapeleka misonkho tsiku ndi tsiku koma mukulephela kukonza zimbudzi, kuchotsa zinyalala mumisika yambiri mumaboma ambiri mdziko muno. Go hard wena Karonga. Ndalama zathu za matikiti zikupita kuti.

Mbanangwa
9 years ago

Fighting for my rights, do not step on my toes!

Emmatuwa
Emmatuwa
9 years ago

Amalawi mwafika penapake kodi ufulu wa democracy ndi umenewu osalipira msonkho
Mavenda inu ndi akuba mukufuna dziko lino likhale mu umphawi. stupid Venda pay tax nowwwwwwwwwwwwwww

Winnie phiri
9 years ago

More fire ma vendors aku Karonga. These assembly officials does not consider vending as a proffession, and yet they are renting in our houses. Ur friends in Kronga main market have shown them a yellow card. Next is Rumphi main market. All officials shall be shown a red card. They are so corrupt.

Pwiyapwiya
Pwiyapwiya
9 years ago

Tawapaseni boma lawo azikana kupereka misonkho awone ngati dziko lawolo lingazAyende lopanda tax.Zindere zakufikapo…

Musa Kilimanjaro
9 years ago

its the poorest of the poor who always suffer

Read previous post:
Matindi FM promises match ball to hat trick scorers: Malawi TNM Super League

As the 2015 TNM Super League is about to kick off, private owned Matindi FM Radio has said it will...

Close