Email a copy of 'KB inflict Nomads major title blow: Malawi TNM Super League' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

48 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Wanga ndi yemweyo
Wanga ndi yemweyo
8 years ago

Pepa neba. Komabe uchitepo kanthu, ukutichititsa manyazi. Nanga ungokhala pachinyezi pomela china chili chonse? Mwina utayenda mwa anthu kuti uwone vuto ndi chiyani. Nanga nkutani?

skillz
skillz
8 years ago

bb wamkaka tikumwa hihih sorry neba

Cathbert catrarakillers
Cathbert catrarakillers
8 years ago

Bt nomads steal remain nomads

fredinho mizelo
fredinho mizelo
8 years ago

chikho chili m’manja a bb dats all.

fredinho mizelo
fredinho mizelo
8 years ago

nyerere womwewo kuti wawa!!!

UNECA
8 years ago

Ngati simumaluza intercity mudatenga shame on u.

UNECA
8 years ago

Which team this yr won the cup, is manoma why not agd team where were u? u lost on intercity shame o u!?

UNECA
8 years ago

Komano kumayankhula bwino ntchito ilipo imaluza madrid osati kuluza noma ndiye kuti zachilendo masiku sakoma onse komanso tikaluza kumavomereza inu mukati amakuberekani ref how many penaltiens u hv given through favour of ref.

nampuzeni
nampuzeni
8 years ago

Nyelele zinali kale, pano iiiiii!……

Mbolo Sidwala
Mbolo Sidwala
8 years ago

Pepa neba. Paja iwe umadalira games in hand, tye nazo usova. How many games in hand watsala nawo? One thng u must do: either upepese game anakubereka ref ija against eni mpira pa flames pano or usinthe home ground. Apo bi, sudzawina game pa Kamtsitsi stadium. Malangizo aulele awa, ziri ndi iwe kuwagwiritsa ntchito kapena ayi. Red lions ikukunkhundidwa lero ndi mapale, tsoka ndi loti idzabwezera mkwiyo pa iwe mu kota fainolo ya Std Bank unless umupemphe Walter kuti akusinthire venue.

Read previous post:
Deliverance is the children’s bread

It is God’s intention that His children must be free from all powers of the enemy. There are so many...

Close