Email a copy of 'Kumbatira booted out as MACRA boss' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

48 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
PHODO
PHODO
8 years ago

WELCOME BACK BOSS YOU HAVE STAFF WELL FAIR AT HEART LULULULU MPC

Nankhoma
8 years ago

A president anthu wokoma mtima koma ali a seventhday ngati Kumbatira simumaona osati zinazi koma pokhapo pobwezela abwana athu ndiye mwachita bwino zinthu zinaima a president Mulungu akudalitseni tinaphinjikatu ife

Super Shake Maheu
Super Shake Maheu
8 years ago

I agree that “re-deployed” should be the title and not booted; choice of words there Nyasatimes!!! Anyway – To everything there is time. China Chili chonse chimachitila ubwino kwa ana ake aMulungu.! Tidzazindikira bwino patsogolo ndithu. We just hope that the politics being played here will not end up very badly for those that are playing it. For AK – You are better of working at a place where you are loved and appreciated than being at a place where there is too much politics and too many bosses. All the best, – your MPC family is waiting for you.!!

chitsilu
chitsilu
8 years ago

zoona iwe itaye Driver mpaka Hearing chifukwa ngalimoto mwasowa Bablegum muwili, atadya ali ana ako ofuntha aja…..?like father like kids…get out…chindele chakufikapo….kkkkkkkk

malizani
malizani
8 years ago

itaye itaye……iiiiiiii.!…munthu oyipa iwe ine sindinaone…koma kwanu anthu samakudaula…..?? ayi its too much….anthu oyipa ngati inu anatha mmalawi muno ndipo nkutheka wasalapo wekha…..change yo life please,ndipo ndiwe munthu ozikonda ngati nzimai…shame on u….ndipo uchite manyazi,uthakhala wina waumunthu ukanazimvela chisoni……ndipo usasanzike uzachitisidwa manyazi,zipitani mukafike bwino ndipo usazabwelenso.olo kuzayenda sitikukufuna kukuonanso umatinyansa mmansomu….welcome back our good boss kumbatira itaye is not even harf the man u are…..he is just a small boy…u are a gentleman Andrew.

Nankhoma
8 years ago

Bwerani boss tikulandirani ndi manja awiri kanthawi komwe munachoka zambiri zachitika timapemphera kwa Mulungu day in day out kufunsa kuti bwanji wachotsa inu kutibweretsera zinalipozi koma tamuona Mulungu akuyankha pemphero lathu ndikudandaula kuti mukabwera simuzapeza zinthu mmene munazisiira chifukwa palibe chomwe chimayenda ma customer munasiya aja anatithawa ataona mmene amachitidwa handle kunalibe macheza pa wailesi zina mwazomwe munayamba abwana anthu ambiri apangidwa ma hearing ambiri achotsedwa ntchito abale a mabwana ndiye alembedwa recruitment amapanga okha a itaye HR inasiya kugwira ntchito yawo tinafatu abwana koma pano taukanso Mulungu alemekezeke

PRINCESS
8 years ago

Let itaye go he was plotting down fall of MPC

HUle weniweni
HUle weniweni
8 years ago

awa amanyenga mkazi wa neba wawo kumaona ngati udolo osadziwa kuti neba wawoyo ali very connected. wawanenera kwa HE ndi izi zathera umuzi.

juviyo
8 years ago

Tikufunilani zabwino zonse ku new position, khalanibe odzichepetsa ndi osadzikweza pa udindo wanu a Kumbatila ndi banja lanunso. Your wife is also a humble lady both at work and home.

May God bless you both

mabvuto
mabvuto
8 years ago

koma chonde a ACB bwerani ku post office muzafufuze anthu onse amene alembedwa ntchito ku post office munthawi ya itaye, its nepotism at its best by this gentleman called itaye, zikutiwawatu, this is bad post office si ya mtundu umodzi, koma itaye kumamangisa anthu chifukwa choti ashota ndalama yochepa, ndiu usatana umenewu,bwanji munthu kungomuchosa ntchito osati kummanga becosz of very little shortage, welcome andy

Read previous post:
Illovo Malawi announces uniform sugar prices

Illovo Sugar (Malawi) Limited has announced uniformity in sugar prices across the country. Consumers will pay K534 269.20 per metric...

Close