A president anthu wokoma mtima koma ali a seventhday ngati Kumbatira simumaona osati zinazi koma pokhapo pobwezela abwana athu ndiye mwachita bwino zinthu zinaima a president Mulungu akudalitseni tinaphinjikatu ife
Super Shake Maheu
8 years ago
I agree that “re-deployed” should be the title and not booted; choice of words there Nyasatimes!!! Anyway – To everything there is time. China Chili chonse chimachitila ubwino kwa ana ake aMulungu.! Tidzazindikira bwino patsogolo ndithu. We just hope that the politics being played here will not end up very badly for those that are playing it. For AK – You are better of working at a place where you are loved and appreciated than being at a place where there is too much politics and too many bosses. All the best, – your MPC family is waiting for you.!!
chitsilu
8 years ago
zoona iwe itaye Driver mpaka Hearing chifukwa ngalimoto mwasowa Bablegum muwili, atadya ali ana ako ofuntha aja…..?like father like kids…get out…chindele chakufikapo….kkkkkkkk
malizani
8 years ago
itaye itaye……iiiiiiii.!…munthu oyipa iwe ine sindinaone…koma kwanu anthu samakudaula…..?? ayi its too much….anthu oyipa ngati inu anatha mmalawi muno ndipo nkutheka wasalapo wekha…..change yo life please,ndipo ndiwe munthu ozikonda ngati nzimai…shame on u….ndipo uchite manyazi,uthakhala wina waumunthu ukanazimvela chisoni……ndipo usasanzike uzachitisidwa manyazi,zipitani mukafike bwino ndipo usazabwelenso.olo kuzayenda sitikukufuna kukuonanso umatinyansa mmansomu….welcome back our good boss kumbatira itaye is not even harf the man u are…..he is just a small boy…u are a gentleman Andrew.
Tikufunilani zabwino zonse ku new position, khalanibe odzichepetsa ndi osadzikweza pa udindo wanu a Kumbatila ndi banja lanunso. Your wife is also a humble lady both at work and home.
May God bless you both
mabvuto
8 years ago
koma chonde a ACB bwerani ku post office muzafufuze anthu onse amene alembedwa ntchito ku post office munthawi ya itaye, its nepotism at its best by this gentleman called itaye, zikutiwawatu, this is bad post office si ya mtundu umodzi, koma itaye kumamangisa anthu chifukwa choti ashota ndalama yochepa, ndiu usatana umenewu,bwanji munthu kungomuchosa ntchito osati kummanga becosz of very little shortage, welcome andy
WELCOME BACK BOSS YOU HAVE STAFF WELL FAIR AT HEART LULULULU MPC
A president anthu wokoma mtima koma ali a seventhday ngati Kumbatira simumaona osati zinazi koma pokhapo pobwezela abwana athu ndiye mwachita bwino zinthu zinaima a president Mulungu akudalitseni tinaphinjikatu ife
I agree that “re-deployed” should be the title and not booted; choice of words there Nyasatimes!!! Anyway – To everything there is time. China Chili chonse chimachitila ubwino kwa ana ake aMulungu.! Tidzazindikira bwino patsogolo ndithu. We just hope that the politics being played here will not end up very badly for those that are playing it. For AK – You are better of working at a place where you are loved and appreciated than being at a place where there is too much politics and too many bosses. All the best, – your MPC family is waiting for you.!!
zoona iwe itaye Driver mpaka Hearing chifukwa ngalimoto mwasowa Bablegum muwili, atadya ali ana ako ofuntha aja…..?like father like kids…get out…chindele chakufikapo….kkkkkkkk
itaye itaye……iiiiiiii.!…munthu oyipa iwe ine sindinaone…koma kwanu anthu samakudaula…..?? ayi its too much….anthu oyipa ngati inu anatha mmalawi muno ndipo nkutheka wasalapo wekha…..change yo life please,ndipo ndiwe munthu ozikonda ngati nzimai…shame on u….ndipo uchite manyazi,uthakhala wina waumunthu ukanazimvela chisoni……ndipo usasanzike uzachitisidwa manyazi,zipitani mukafike bwino ndipo usazabwelenso.olo kuzayenda sitikukufuna kukuonanso umatinyansa mmansomu….welcome back our good boss kumbatira itaye is not even harf the man u are…..he is just a small boy…u are a gentleman Andrew.
Bwerani boss tikulandirani ndi manja awiri kanthawi komwe munachoka zambiri zachitika timapemphera kwa Mulungu day in day out kufunsa kuti bwanji wachotsa inu kutibweretsera zinalipozi koma tamuona Mulungu akuyankha pemphero lathu ndikudandaula kuti mukabwera simuzapeza zinthu mmene munazisiira chifukwa palibe chomwe chimayenda ma customer munasiya aja anatithawa ataona mmene amachitidwa handle kunalibe macheza pa wailesi zina mwazomwe munayamba abwana anthu ambiri apangidwa ma hearing ambiri achotsedwa ntchito abale a mabwana ndiye alembedwa recruitment amapanga okha a itaye HR inasiya kugwira ntchito yawo tinafatu abwana koma pano taukanso Mulungu alemekezeke
Let itaye go he was plotting down fall of MPC
awa amanyenga mkazi wa neba wawo kumaona ngati udolo osadziwa kuti neba wawoyo ali very connected. wawanenera kwa HE ndi izi zathera umuzi.
Tikufunilani zabwino zonse ku new position, khalanibe odzichepetsa ndi osadzikweza pa udindo wanu a Kumbatila ndi banja lanunso. Your wife is also a humble lady both at work and home.
May God bless you both
koma chonde a ACB bwerani ku post office muzafufuze anthu onse amene alembedwa ntchito ku post office munthawi ya itaye, its nepotism at its best by this gentleman called itaye, zikutiwawatu, this is bad post office si ya mtundu umodzi, koma itaye kumamangisa anthu chifukwa choti ashota ndalama yochepa, ndiu usatana umenewu,bwanji munthu kungomuchosa ntchito osati kummanga becosz of very little shortage, welcome andy