Email a copy of 'Lilongwe 'block leaders' march to demand council directors removed' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Lilongwe 'block leaders' march to demand council directors removed' to a friend
Ground work has begun ahead of the construction of a multi-million dollar Daeyang Luke Teaching Hospital, a facility that is...
Lilongwe City Assembly, mukachedwa, tithana nawo tokha anthu amenewa. These block leaders are day light robbers, tiyamba kuwaotcha tsopano
If thses pepole want to be called chiefs let them go to their villages and cry for chieftency there. cities and towns are not villages, we do not need these self proclaimed blockleaders or “chiefs”. These people are a nuisance during funerals to the bereaved. they want to be treated like kings, they also steal part of the donated condolence contributions. If they have nothing to do let them start farming.
Amasowetsadi mtendere amalawi mpakana kumalanda malo anthu mkumagulitsa. Apite kwao akakhale mfumu kwao osati mtauni
#1, you are right. Ndi anthudi okuti chochita alibe, ndiye amaona kuti kukhala block leader ndiye kuti zawo ziziyenda. And moreover anthu ake monga gulu laku Lumbadzi ndimbuli zokhazokha zosamva upangiri, odwalika, komanso mfiti. Ntchito kulimbana ndi eni mtunda. Asiyeni mafumu adzitilamula bcoz iwowo ndamene aliovomerezeka ndi malamulo adziko lino. Mu constitution yadziko lino mulibe zama block leader.
Kkkkkkkkkkkk, most of these block leaders are retired civil servants who are no longer recognised in their home villages and can not go and settle there, they are rejects. Examples are people like Mr Chikope at Bwemba or area 46, ntchito ufiti wakwao ku Mocambique basi, Kumalodza anthu pa line. I support govt, these idiots have to go, amasowetsa mtendere