Email a copy of 'Lilongwe city council tells block leaders to go to polls' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Lilongwe city council tells block leaders to go to polls' to a friend
Malawi’s media giant Times Group has criticised the Democratic Progressive Party (DPP) government for its “failure to see what people...
Awanso mmalo moti azipanga concentrate on real issues akupanganga prioritize za zii! I am yet to find out what convinced councilors to elect as you capital city mayor. Another big flop.
Kodi inu a LL City council munatifunsa anthu amene timakhala ndi ma Block Leader? Kumeneko ndi kusokoneza tinamenya tokha nkhondo yolimbana ndi mafumu akhoza ndipo pano tili pa ufulu. Komanso ndinamva kuti anthu azichita kampeni (campaign) “Kodi ufumu amachitanso kampeni.Musiyiretu khalidwe lanu ladyera mukulephera kupanga zitukuko mmadera koma busy kulimbana ndi ma block leaders.