Email a copy of 'Lilongwe man chops wife's hands, gets vigilante justice' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

72 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
kasisi
kasisi
9 years ago

Koma zinazi aaa kusowapo comment

Chilungamo.
9 years ago

apapa ayi mwamuna waonjeza. Kodi akazi muziwapanga chonchi? Kulakwatu uku. Kodi ngati zavutitsitsa bwanji oxangosiyana? Hey u man wait ur jehena!

chifundo
chifundo
9 years ago

This is wat we call nkhaza zophelatu, how can a real loving husband did this to a woman whom he considers a wife? Ufiti ndi umene wakula for sure. Malawians are known to be peace lovers koma izi zikutionongela CV as a nation at large, these pple need to b given coporal punishement

Odala Ochibwe
Odala Ochibwe
9 years ago

Bamboyu Waonjeza Koma Nkhanzazi Zikumachitika Mbali Zonse Amuna Ena Amakokedwa Maliseche Koma Samanena Choncho Ndipofunika Pakhale Lamulo Lokakamiza Mabanja Amene Amakhala Ndi Mikangano Kawiri Kawiri Azitha Chifukwa Zimakhala Kuti Nkhani Zawo Sizikutha. Kutero Nkhanza Zoterezi Zikhoza Kuchepa.Komanso Malamulo Alipo Amakondera Akazi Zimenezi Zikupangitsa Akazi Ambiri Kumapanga Mwano Kwa Azimuna Awo.Pelekani Ufulu Wokwana Kuti Amuna Azikhala Omasuka Kunenena Zomwe Amakumana Nazo M’mabanjamu!

Petros
Petros
9 years ago

Real satsanism

Frazer Pondiya
Frazer Pondiya
9 years ago

Lucky of humanity! Shiiiii up to hands cut off? GOD will punish u

Mong'onyolani
9 years ago

Apa cikuonmetsa kuti mwamuna ndi mbola koma mkazi ndiokongola….jelasi yakula kwa mwamuna. Anthuni Muonetsetsa

nkhedu
9 years ago

gud move

malawian
malawian
9 years ago

Mchdwa ameneyo

Austin Mussa
Austin Mussa
9 years ago

Owerenga khala maso Yesu Ali pafupi

Read previous post:
Britain won’t resume Malawi aid: Resolve cashgate from 2005 – House of Lords

Malawi’s biggest donor, Britain will not be able to resume aid support  until the  government clamped “firmly down on corruption...

Close