Email a copy of 'Lilongwe man chops wife's hands, gets vigilante justice' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Lilongwe man chops wife's hands, gets vigilante justice' to a friend
Malawi’s biggest donor, Britain will not be able to resume aid support until the government clamped “firmly down on corruption...
Koma zinazi aaa kusowapo comment
apapa ayi mwamuna waonjeza. Kodi akazi muziwapanga chonchi? Kulakwatu uku. Kodi ngati zavutitsitsa bwanji oxangosiyana? Hey u man wait ur jehena!
This is wat we call nkhaza zophelatu, how can a real loving husband did this to a woman whom he considers a wife? Ufiti ndi umene wakula for sure. Malawians are known to be peace lovers koma izi zikutionongela CV as a nation at large, these pple need to b given coporal punishement
Bamboyu Waonjeza Koma Nkhanzazi Zikumachitika Mbali Zonse Amuna Ena Amakokedwa Maliseche Koma Samanena Choncho Ndipofunika Pakhale Lamulo Lokakamiza Mabanja Amene Amakhala Ndi Mikangano Kawiri Kawiri Azitha Chifukwa Zimakhala Kuti Nkhani Zawo Sizikutha. Kutero Nkhanza Zoterezi Zikhoza Kuchepa.Komanso Malamulo Alipo Amakondera Akazi Zimenezi Zikupangitsa Akazi Ambiri Kumapanga Mwano Kwa Azimuna Awo.Pelekani Ufulu Wokwana Kuti Amuna Azikhala Omasuka Kunenena Zomwe Amakumana Nazo M’mabanjamu!
Real satsanism
Lucky of humanity! Shiiiii up to hands cut off? GOD will punish u
Apa cikuonmetsa kuti mwamuna ndi mbola koma mkazi ndiokongola….jelasi yakula kwa mwamuna. Anthuni Muonetsetsa
gud move
Mchdwa ameneyo
Owerenga khala maso Yesu Ali pafupi