Email a copy of 'Lipipa conceeds Bullets on knifedge over Nyasa takeover' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Lipipa conceeds Bullets on knifedge over Nyasa takeover' to a friend
Malawi Communications and Regulatory Authority (Macra) top management has since Friday been working under pressure to correct scores of illegal and...
ine kudabwa ! Kodi inu achina Fote… pamene BB imapanga dealyi inu munalikuti? a Malawi vuto ndilimenero… mumafuna munnthu alephera kenako inu muzioneka ngati a nzeru ! UMENEWO NDI UFITI ! SHUPIT ! basi ife tipitilira ndi NBB yomweyo inu kagwereniko uko ma failed leaders !
amphawi awa analowera kuvutika
ZIKATERO ZAYAMBIKA TSOPANO
Maule and fake ceo. Mwasamba matope. Matsotsi akupusitsani
Mr Lipipa please be serious and stop the nonsense.Who can believe you now after all this time? You were part of the whole process and now you want to appear as if you are an angel. sour grapes!
Kodi a Lipipa bwanji? Vuto lanu ndi chani? Nanga a Harold Fote, mukati anthu akufuna adziwe, anthu ake ndani? Kodi chomwe mukuona inu kuti sichikuyenda bwino ku Maule ndi chani? Kodi ndi inu a Wanderers eti? Akutumani kuti nanu muyambitse mpungwe pungwe ku Bullets popeza kwao silikuyenda? Palibe sapota wa maule yemwe akudandaula pano kupatula inuyo mwina, ndikutitu mwina ndi aku banja lanu. Chomwe Maule timachifuna tachipeza tsopano chifukwa panopa; 1. Ma player kulambalala 2. Timu ikuyendetsedwa mwa ukadaulo osati ngati chipani 3. Tsogolo la team ikuoneka osati za manyakazi ai. 4. Zoyambana yambana ngati si ife atimu imodzi tinasiya… Read more »