Email a copy of 'Maize prices rise by 37% in Malawi -Admarc' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Maize prices rise by 37% in Malawi -Admarc' to a friend
A 13old Mtisunge Kamphale has pleaded with international organizations attending the 70th United Nations General Assembly in New York, United...
komabe nzeru za munthu zalephera kutetsa njala, kwa anzungu nawonso akulephera kukonzanso nyengo yowonongeka, pakibe ali ndi nzeru.
Malawians suffer because of poor choice of leaders.The yard stick for electing somebody is names,titles and tribalism.They don’t look for policies.So don’t cry of hunger.Pitala and his entourage are feasting on xxxl chicken and chips at Hilton hotels washing down with some expensive juices.Koma Ndiye mufotadi ndi njala kamtundu kopusa ndipo kosamva.Koma ndiye mukhauladi ndi mlomweyi mpakana 2019.
Tikapita ku joni akutiphako tikhale kwathu kuno mbeu dzikupysera m’munda nanga tipange chiyani ife anthu anu ambuye. Atsogolerinso zoti kulinjala sakusamala ai akuti bola iwo akukhuta. M’malo mugula chimanga akuononga ndalama kutengera anthu kuka nyada kunja votiyanga ija ineeeeeee!!. Ndinabetsa
Dziko langa lija ine talakwanso chiyani nanga kodi chalangochi chikufikira ifenso tikhululukireni YEHOVA, ndikudziwa masatanic ndi amene akupangitsa mcholinga choti anthu avomereze kuti anthu akhazikike pokwatirana okhaokha nchokinga akuti tililandila thandizo lo chokera kwa iwo oyipayo Mulungu wangatu akuona athanananu
I think Malawians are the most stupid people on this planet earth. It’s normal when supply is low, demand is high, price increases, simple. If we had bumper harvest as a nation, the price of a bag of maize would not have risen simple!!!
NDE TITANI PAMENEPA MOYA CHE MUTHARIKA PANGANIPO NGATI MAMUNA APA ZISANADEPO
kaya
Ife tidanena kuti awa mbuyache aabwelesanjala kumalawi kuno,sizimenezonanga…titoona kumenezitatheleko!
Its high time the Mw gvt should think of removing fertilizer subsidy, becoz we are losing out 50 billion Kwacha on fertizer subsidy but its not giving us the intended results unlike removing serving K22 million for JCE printing of certificates
kkkkkkkk malawians too much crying. Nthawi munalinayo yokoza dziko, mumafuna chimanga 4. Lero mwaziona. Mulungu akulangeni kwambiri mufe ambiri ndi njala imene mwina muphunzira kusankha bwino. Tsogoleri akakhala wabwino dziko limakhala lamadalitso. Koma iri mavuto ngosayamba tilira.