Email a copy of 'Makande arrested in Malawi ‘cashgate’: Turns himself to ACB' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Makande arrested in Malawi ‘cashgate’: Turns himself to ACB' to a friend
The House of Lords in Britain will debate a Motion on aid to Malawi on Thursday, Nyasa Times learnt in...
apanidwe mpaka abweze zonse,amine kuti mfiiiiii!
Wawa Bammbo Makande!! Lyo!Lyoo!lyoooooo! PP woyeee! Mwana weniweni wa mayi chiongolelo ameneyu. WATCH OUT GWENGWE!!
@ Blues,let us not be carried away with our imaginations. German has given almost 10billion kwacha to audit 2009-12 period when these audit querries arise. Germans are not fools to play silly games and throw about monies. Pati biii pali munga. Those of 13billion are facing it now. The 92b culprits wish time stands still to avoid their destined fate.
Ogonakukhomo kosatseka akulumidwa ,udzudzu kundende kikikikikiki ine ndiri mu net yanga ndi akazanga pheee ,
Inu ACB, musamaulule m’mene mukuchitila ma “investigation” ai. Kwenikweni za JB. Musapuse nazo; mwina akamva, sazabwela. We want her in Zomba Maximum!
Ndale zakumalawi zimenezo….DPP ikadzachokanso nkhani za cashgate zidzakhalaponso
Mukunama , Makande? Makande wake uti? Bodza lankunkhuniza. Nda amuna amenewa ogona kukhomo kosatseka, sangamangidwe.
ndiye mwati Makande ndi mamuna sangamangidwe? Ngati muli ndi makutu mwina by now mwamva
Put cashgaters in a cooler without mercy but next be 92 billion cashgaters dead or alive. All must face justice & make sure they return all the cash to government. Malawians be careful the returned cashgate money can be cashgated by DPP since our focus is only on PP. Mark my words!
Tiye nayoni anasimbwa agalu amenewa. By the way, where is JB THIS TIME ROUND? HAS SHE COME BACK FROM WHERE SHE WENT TO BEG AFTER THE CASH GATE STOPPED?
a makande ndiye sizimakuthelani, chaposachedwapa munamangidwanso pa milandu ija ya ‘kangwazi’ ndi mbaza zomwezi za chilomwezi pano ndiye zikukakamirani koopsya mukathera konko basi!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!