Email a copy of 'Why Malawi Agriculture Minister George Chaponda too must go over 'maizegate'' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

8 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
misozi banda
misozi banda
7 years ago

MInister wa ziphwisi idiot iye amakapwisila kuti. nditi amangonunkha zifwenthe pakhala iye,mwina amaphwisila mmapilikanilo. kucititsamanyazi ziko lose la pasi kuziwa kuti anthu asamangopwisa palipose BBC,CNN, ndiye mmene timadyela ntolilo nyemba mbatata makaka ndi nandolo, ziphwisi zakezo !!!!! ndiye tisamatuluse gas.
lunyasa cinkhope nyalugwe ndi pitala wakoyo

misozi banda
misozi banda
7 years ago

uyu ingobayani ndi muvi bwa???? Caponda akamacokera kosamba/kuphikidwa ku mazambici amazakotu mma bandakuca. misonkhano ya usiku yoti aononge dziko. awa kodi nde nda acilungamo???????????????? uyu tikungomuyangana now pali nkhani iyi VAKABU lamulo la 1934 and masiku osewatu bwanji osaliunika kale lomwelo????????????? pano mwacotsa ma ulemu aanthu. mma location ma gate thoo komatu coseco mma locationmo muli ma lawyer , anthu odziwa za malamulo. a polisi mwamanga anthu ambili. lamulo lokomera anthu a magalimoto. ma hardcore mbava amayenda mmagalimoto. ena amagalimoto mbanda zenizeni malamulo aazaungu(azungu atiuza) pano nde titsekule milandu pomatimanga kuticotsera ufulu oyenda usiku. A khoti masulani bwinobwinotu apankhani yatalika… Read more »

jone
jone
7 years ago

CHAPONDA SABA

Papa Chalo
Papa Chalo
7 years ago

Once Chaponda is arrested he will reveal more evil deals they did in the past with Peter. No wonder Mutharika
is afraid to fire Chaponda. 7 Ministers posachedwapa mumva m’bebe. Mulungu atimenyera nkhondo.

Ma floods munabweretsa ndi inu? It’s GOD. Chaponda has revealed himself in the process of serving flood victims.

Mupita Nonse Mbava inu.

RICHMAN
RICHMAN
7 years ago

A Kasakula apa ndiye mwanena chilungamo zampweteka aphulika ndipo wakwiya nanu ndi mfiti

koma abale inu eeh
koma abale inu eeh
7 years ago

Koma iwe George Kasakula: umandibowa bwa? (GK: I can’t believe I spent a minute reading your column to discover nothing new!) Columnists worth the honor should come up with revelations, not just regurgitated opinions: because columnists are supposed to have connections to enviable and reliable sources. Sources that reveal accurate information we are hungry for. Do you have any such sources, really? You seem to call for Bwana Chaponda’s exit based on your opinion that he is arrogant. (And I can’t believe you brought up the so-called anti-farting law) Not that he is incompetent. The man, in his service to… Read more »

Chambe
Chambe
7 years ago

Koma abale inu eeh. You are just spot on! Can’t agree more.

Yankho Yapuwa
Yankho Yapuwa
7 years ago

In as much as the issues raised in the article maybe a bit ‘regurgitated’, couple of premises here aren’t in order. 1. Even though Admarc was sorely responsible for the procurement, a deal that big and of such significance would require the scrutiny from the responsible minister and that means Chaponda. The guy at admarc has been relieved of his duties. DPP supporter or not you have to acknowledge the hard truth that for a proper investigation the minister has to step aside. 2. To the best of my little knowledge I thought cases involving some aspect of fraud are… Read more »

Read previous post:
Blantyre Mayoral polls: Chalamanda favourite of ‘cityzens’, DPP’s Ngalande eye post

The tension for Blantyre City Mayor’s elections on Monday is heating up with current Mayor, Noel Chalamanda facing opposition from his deputy...

Close