Email a copy of 'Malawi angers UN over misuse of HIV money, risk losing Global Fund help' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

81 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
NYATWA MJ
9 years ago

Koma Pitala mpakana zina kupatsako Gyan

Poor malawian
Poor malawian
9 years ago

a Malawi kusamva komanso kusachedwa kuiwala…dont be cheated kuti ndi amayiwa ndi Mamunayi .musaiwale Mkuluwake amachita chimodzimodzi kumatenga ku escom,malawi savings bank and many more tonse tinawona komanso kumva .mkaziyi wabwera liti kuti akapeze mphamvu zoterezi ….to me i rule it out the its Mrs, its Mr himself……kugwiritsa ntchito udindo molakwika…..kukagwiritsanso ntchito molakwika.

Tiyendamo
Tiyendamo
9 years ago

UNAIDS should not try to be holier than thou. They have also been milking NAC through their bogus Protect the Goal Campaign Project. They took money for Asamoah Gyan and also for a number of Ministry of Youth Programmes. Copies of the payment vouchers are there. NAC should respond to this if it is not true. The UNAIDS Commission Summit hosted by Joyce Banda also took over K50 million. Akhale chete amenewa!

Nchengeti
Nchengeti
9 years ago

The money must be paid back.
BEAM = Cashget

Munthu wa Mulungu
Munthu wa Mulungu
9 years ago

Za AIDS zokhazi bwezani. You have crossed the line. Apo bii! timatcha.

residence of Manase
9 years ago

zoona inu a nac mukapeleke 5milion ku beam,mwaona global fund will hold its funding,dpp ndiyakuphadi pano mufuna muphenso anthu oti akuzigwirira ntchito ali ndi hiv mukupeleka cash ku nisb kuti chani ku mulakho why giving that stupit grouping anthu ozikonda,ndalamazo mubweze ngati mukutumikila anthu refund,koma ngati mutumikila zinyama zidyeni anthu tife amene tili pa treatment,agalu angulu inu simunati pitala ali ndi ndalama bola amai or mukanamusiya Chakwera alamulire bz is the one tikudziwa kuti anawina,zonsezi ndi mkwiyo wa Yehova zinthu zikudula daily

Mong'onyolani
9 years ago

Kukhala mai sichifukwa.Boma la Joyce Banda linayesetsa kufukula cashgate ndikuyamba kuzenga milandu mbala zonse. Peter apa ndiye mwaonjedza mpaka kuba ndalama za Global Fund? Musova

Mayi Bwampini Muthalika
Mayi Bwampini Muthalika
9 years ago

Zochitika Ku malawi zingakupange munthu kusiya chichrisitu ndikuyamba kutukwana. Nanga zoona mabungwe atatuwa achita pamenepa si cashgate imeneyi. Kodi a Dausi ndiye kuti mukudwala edzi limodzi ndi Mayi Bwampini? Bwanji mukufuna kusokoneza ntchito za edzi mdziko.

wakukayawakukaya
9 years ago

Kangaroo ndikanyama sangakhale munthu.

Quota system
Quota system
9 years ago

NAC gate

Read previous post:
Shooting our wounded, a tracherous ploy mastered by our army

“If you judge people, you have not time to love them.”-Mother Teresa At any cost an army is supposed to...

Close