Email a copy of 'Malawi army soldier arrested over Indian Hemp' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi army soldier arrested over Indian Hemp' to a friend
Minister of Sports and Culture Grace ‘Obama’ Chiumia has threatened an unspecified tragedy will strike journalist James Chavula who exposed...
fuck the police how can they arrest their fellow motherfuckers yet they do the same sh!t
No37 usova zangokuvuta wakhaula wasowa kokatulira thudzi takoto.
Asogolele anthu adziko kusogolela njira kwa anthu osuta chamba mkumati mungalandile ulemu chocho ???? Mwatani kodi asilikali anthu. Simungationesele zisanzo zabwinoyi kt enafe mkusinthikaaa ???????
Useless, osamusiya bwanj, chamba ndi deal simudziwa
Since 2014 three soldier kugwida ndi chamba, 54 senior officers and soldiers kuthetsa maukwati ndi akazi awo, 10 families senior officers kunyenga akazi anzawo, one akupanga zimenezi akuti cream ya commander Mr Tactic Ig Maulana. The commander is pretending as if he doesnt know but he knows malamulo therefore akuopa kuchosa ntchito anyamata ake. Waona iwe Klausi zomwe unatipasa kuno ku amry. Nzako Maulana anapha 5 soldiers whom he forced to swim in lilongwe river during rainy season and they died because of his stupid tactics. so do you think he can command the whole army and maintain displine. Saulos… Read more »
A army ku delera lamulo munya muona nobody is above the law mnzanu ODELERA waluzatu ntchito azikalima chamba chakecho
Kaombe roadblock get ready anytime as we will be going to Moyale from KB or MAFCo tidutsa lakeshore,muona zosaona mwaonjeza.Ulemu ukuchepa sopano ndiye tisovepo ziwiri sitatu ndi inu…anytime soon just get ready
kudya kumeneko
Mumati akudyereni kuchipatala?
NO WHY ARRESTING HIM? MESA CHAMBA AMASUTA ASILIKALI? No free him