Email a copy of 'Malawi church says stop calling it 'Ass of God'' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi church says stop calling it 'Ass of God'' to a friend
Malawi Congress Party (MCP) says the ruling Democratic Progressive Party (DPP) has launched a terror campaign in the Nsanje Lalanje...
Hahahahaha!
or otherwise pemphani moderator to withdrawal your comment here
A Ndyomba, ngati mulibe zokamba just keep quite. Ndi za Mulungutu izi. Don’t sin jockingly. Pamenepo mukumutukwana ndani? Lapani ngati mumadziwa kapena kumvapo za Mulungu.
Zubwera mochedwa. Nawo ma yo aku USA kusocheletsa anthu too much
Kodi azibusawa ma PHD akumawatenga kuti
Kikikiki! koma iwe Muheya, mpaka ‘Asses’ for the church’s faithful!
Matako a ambuye kkkkkk
kkkkkkkkkk hahahahahahaha aise Ndyomba its more like NYERO la MULUNGU! Iwe ukudana ndi comment ya Ndyomba matako ako. Kodi nkhaniyi walemba ndi Ndyomba? kodi mmayesa ngati Mulungu wanuyo ndi choopsezera anthu eti? Kodi mukudziwa kuti dzina looti mulungu kuno ku SA limatathauza Nzungu, kapena kuti munthu oyera khungu mchiyankhulo china? Kuti muone ndi mzungu yemweyo amene anabwetretsa baibulo kutiuza kuti kuli mulungu ndipo mulunguyo ndi oyera khungu. ndi kupanga anthu ambiri kukhala a khirisitu, ndipo a khiririsitu ndi amene ali very judgmental pano pa dziko lapansi. Ngati siukuchita zomwe akukhulupilira iwowo amati akuti ukupsa ndi moto olo ukaonongeka. koma ukachita… Read more »