Email a copy of 'Malawi couple arrested for theft of goats, maize' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi couple arrested for theft of goats, maize' to a friend
TNM Super League rookies Dedza Young Soccer have put strict measures on their defender and captain Chisomo Mpachika to Bullets...
Zaziiiii
Mbuzi yinatsalira mkholamo ndiyomwe yalemba bwiribwishi apa.
Zinayamba ndiboma kuba ndalama.mukuwagwira kuti alakwa
Ulesi too much achawa mxiew
mbuzi amaphera kholamo zinali zawo kodi apolice abalaka ndinu mashasha kwambiri anthu akatenga katapira mumalowerera ngati mene amapasana ndalamazo mumakhala mboni ndinu mwana anamuwotchayo wawo pobwera kupolice kumene munawamanga apeza nyumba mopanda kathu mumati adya chiyani agalu zimangani anthu chocho ngati mbuzi koma siku lina muzadulidwa mbolo apolice anyani
Koma asakhwi inu, mudzadziwa liti kulemba chizungu cholongosoka???? Mukutichititsa manyazi….
Akanakhala mtumbuka mukanamva ma comments ake….
Koma banja ili anatengana mbava zokhazokha nde mwana analibe kothawira.
Mayi yo nayeso timuotche zala naye amve kuwawa ngati mwanayo
Family of the Year.
This is to advise the Nyasatimes reporter from Balaka to stop publicising trivial issues like this one. Malawi is a big society and there are a lot of important issues to be shared and not of this type. Recently, there has been a lot of coverage of negative things about people of Balaka, but they are good enough to be left out of this important online news post, as most of them are trivial and not in the interest if the public.
a Bushiri apiteko akachotse mizimu yoyipa