Email a copy of 'Malawi court convicts man for defamatory Facebook post' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi court convicts man for defamatory Facebook post' to a friend
Malawi Parliament's Budget Committee has come out panting, accusing the ruling Democratic Progressive Party (DPP) of high level corruption in...
Too bad for the poor soul. But he deserves it. He new that he was guilty that is why he is asking for leniency
Feb 21 2017 12:34. zonse zimene zikuchitikazi zikusonyezadi kuti tili mmasiku otsiliza. Onamero
Nkhaniyabwino,Nanga amene akuba ma million aboma osapanga chimodzimodzi bwanji ngati mene mwapangila wapa Facebook,
Za pa Tumbo
Only in Malawi are you not free any other country this would be a civil matter. Libel what harm did did the too reputation.
Malawi legal counsel should immediately appeal this decision.
Just undemocratic and scary someone is jailed for such minor posting.
amangeni!!!
Zili bwino pa Facebook kukumachitapo chibwana kwambiri, khani za bodza bweeee, kumangoipitsa adzanu munya muona mukathera ku Maula. Ena kunyoza president osabwera poyera bwanji? Kunyoza azanu mufinyidwa musiyiretu khalidwe umenewo. Ena mukunyenga heavy amkadzi a Eni ma Facebook mugwidwa ndipo akulangani akhoti. Munaonjedza kuzionera okulakula eti. Am happy
Good lesson to those of us with expertise in fabricating stories and spreading lies…
mxiii
zapanda mchele
back to one party rule
I agree with the learned Magistrate, this case will set a precedence and others will learnt to exercise their press freedom / freedom of speech with full responsibilities.