Email a copy of 'Malawi ex-first lady Shanil, Omar, Lucius on board UTM: Gondwe tells Chilima ‘be our Magufuli’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

39 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Lord of the Flies
5 years ago

magalimoto awa mawaba kuti please? Nsaluzi wagula ndi ndani? Ma ballet? T-shirts? Nanunso ngakuba.

Lord of the Flies
5 years ago

The Chilima movement is tainted by the coming of Msowoya, Jesse Kabwira, Omar etc. People are tired with these thieves breaking away from fellwo gangsters udf and dpp.

kaka ni dada
kaka ni dada
5 years ago

MCP boma kale, izo ndi Ng’oma za dambwe lina, kutekeseka palibe apa. Anthu muli mnyumba imodzi mwabibilamo mwanunkha wina potulukamo aziti ine sinabibilemo nawo. “Namkununkha sadzimva ” Dzuka Malawi dzuka!

Mahule
5 years ago

Loveless not Loveness started her evil business when she dumped her husband in 1996 to marry Yeremia Chihana. Now she is continuing with her bad habit of changing men at will by changing parties at will. Yeremia is a corrupt person through his corrupt estate agency. We should not forget that Chilima himself refused to receive a petition from CSOs which condemned corruption and nepotism among other things.Chilima has failed to condemn the quota system while in government. He wants to look a saint now. He should tell us where he got all the cars that had been paraded at… Read more »

Samuel
Samuel
5 years ago

Oho kuwerenga mbewa ndi michila yomwe. Gwanda adalindichikoka chooooopsa. Panali chani apa. Adaimika makandideti 193 koma adapeza 7 chabe. Nyimbo imene adayimba chitatha chisankho yomweija yotchukayi “ATIBERA”. Chilima wayambakale kuyimba akuti afuna atibere. Nzanunso ankatero kuti afuna atibere koma sizitheka after kuvota “atibera tipita kukhothi. Nanunso pa 22 May pano mudzaimba NYIMBO yemweyi “ATIBERA” Chipani mudalembetsa 2016 UTM zaka zonsezi umamupanga sabotage Peter and you pose kuti ndiwe opemphera ANTHU MULI NDI NSAMBI SIZINGAKUYENDERENI. KHULUPILIRANI MUDZALIRA PA 22 MAY 2019. KUNJA KUNO KULI MULUNGU.

Wisey
Wisey
5 years ago
Reply to  Samuel

Tikulira kale ife ndiye palibe kusiyana ngati obwerawo adzapange chimodzimodzi. Chomwe tikufuna ndichoti ena avinemo m’bomamo. Ngati kuli kuba abe anthu ena tsopano. Inu ngati mukudya nawo za boma lalero dziwani kuti mawa akudya ndi ena. Kodi ndalama za misonkho za Malawi ndi za anthu amodzimodzi?

nyoko
nyoko
5 years ago

There is nothing new here.This is just the result of overpopulation.Everyone wants to be famous,to be cabinet minister
,vice president etc.

Langwani
Langwani
5 years ago

From the look of things , these are the very same regects from these other parties . Most of them sakuwafuna anthu mma dela mwao and sadzawina ma parliamentary seats come May 2019 . And even ma primaries they can’t maintain there seats . Pangani kafuku fuku you will agree with me . Kunali NDA inabwela ndikutentha but it was gone in seconds . Recycled politians basi they will do the same if given a chance . Fisi ndi fisi ngakhale atayenda masana

UTM Boma
UTM Boma
5 years ago

Peter Muthalika ndi DPP mwayiwona launchiyi???????Masamu wochesela ayambikatu,samalani mupakila ku state House ngati mumene Joyce Banda anapakilira 2014!!!

Mfumu yopanda madyela
Mfumu yopanda madyela
5 years ago
Reply to  UTM Boma

kkkkkkkkkkkkkkkk i pray that God grant me life to witness whatever happens.

Spinoza
5 years ago

This is why i dont trust this movement. The same old faces. I like chilima & i believe he is visionary but akumuimbila ng’omawa mmmm azamusokoneza akazawina. Unless azakhale dictator opanga only what convinces him to be wright otherwise atambwali enawa will be giving him stupid pieces of advices

Tate
Tate
5 years ago

Chilima sold his house to a cashgater, Kaliati corruptly acquired minibuses and ACB has another case on her. Callista was paid taxpayers money without working and used to insult US during Bingu’s reign, Masangwi is corrupt and a former cadet leader, Lucius Banda was convicted of forging an MSCE certificate. WHERE IS THE CHANGE HERE? None of these people can bring change to Malawi.

Njazi
Njazi
5 years ago
Reply to  Tate

Can you bring change to Malawi? Actually you can’t because we don’t even know who you are ndiwe chigoba, stop talking nonsense and see how people are suffering in the hands of this so called the government of Malawi.

Chikuli
Chikuli
5 years ago
Reply to  Tate

What is your case Tate

Huwee
Huwee
5 years ago
Reply to  Tate

Chilima is said to be the guy that rigged elections. Is that corruption, Cheating technic thieving Tell me!!

Read previous post:
Zomba MP Nangozo-Kainga in praise of DPP after dumping PP

Zomba Central legislator, Patricia Kainga Nangozo, has said she is home and dry in the ruling Democratic Progressive Party (DPP)...

Close